2 Pedro 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Ndine Simoni Petro, mtumiki ndi mtumwi wa Yesu Khristu.
1 Ayu Simon Peter, Jesu Keriso ana akir wairafin naatu ana tur abarayan.
2 Chisomo ndi mtendere zochuluka zikhale nanu pomudziwa Mulungu ndi Yesu Ambuye athu.
2 Ayu ayoyoyoban God ana manaw ana kabeber naatu ana tufuwamaim nigegewasini, saise God naatu ata Regah Jesu Keriso ana so’ob tutufin etei kwanaso’ob gewas.
3 Mulungu mwa mphamvu zake anatipatsa zonse zofunika kukhala moyo opembedza, potidziwitsa za Iyeyo amene anatiyitana ku ulemerero wake ndi ubwino wake.
3 It ata ma yawas isan God ana fairamaim sawar etei’imak itit. Naatu i taiyuwin ana fair naatu ana gewasinamaim eafit Jesu Keriso’one Kirisiyan anama yawas taso’ob.
4 Mwa ulemerero ndi ubwino wakewo, anatipatsa malonjezo opambana kwambiri ndi a mtengowapatali. Amenewa ndi malonjezo amene amakuthandizani kulandira nawo moyo wa Mulungu, titapulumuka ku chiwonongeko chimene chili mʼdziko lapansi chifukwa cha zilakolako zoyipa.
4 Nati fair ta’imon naatu eomatanen gewagewasih maiyow itit, saise nati siwaramaim iti tafaram ana gurusen kakafih boro kwanahaiw, imih wanatowan anama gewas kwanafarambonen kwanama.
5 Choncho, chitani khama kuwonjezera moyo wabwino pa chikhulupiriro chanu, ndipo pa moyo wabwino muwonjezerepo nzeru.
5 Anayabin iti isan, kwanasinaftobon gewasin a baitumatum tafan kwanaya’abar, naatu gewasin tafan so’ob kwanaya’abar,
6 Pa nzeru muwonjezerepo kudziretsa, pa kudziretsa muwonjezerepo chipiriro, ndipo pa chipiriro muwonjezerepo khalidwe lolemekeza Mulungu.
6 so’ob tafan roumutufuren kwanaya’abar, roumutufuren tafan, baitafofor kwanaya’abar, baitafofor tafan God ana yawas kwanaya’abar,
7 Pa khalidwe lolemekeza Mulungu muwonjezerepo chifundo cha ubale, pa chifundo cha ubale muwonjezerepo chikondi.
7 naatu God ana yawas tafan Kirisiyan ana yawas kwanaya’abar, naatu Kirisiyan ana yawas tafanamaim yabow kwanaya’abar.
8 Ngati zonsezi zikhala mwa inu nʼkumachuluka, zidzakuthandizani kuti musakhale aulesi ndi osapindula ndi chidziwitso chanu cha Ambuye athu Yesu Khristu.
8 Sawar hai ah gagamih i iti kwanabow, naatu kwanabow uma awan nakakaratan na’at, boro nakura’ara’ahi a yan kwanabat, naatu ni’obaiyi ata Regah Jesu Keriso kwanasu’ub.
9 Koma ngati wina alibe zimenezi, ndi wakhungu sangathe kuona patali, ndipo wayiwala kuti anayeretsedwa machimo ake akale.
9 Baise sawar iti men kwanabow a yawas tafanamaim kwanayaya’abar kwa boro mata hinifimabe, ef yok boro men kwananuw. Naatu a yawas atamanin bowabow kakafinamaim kwama’am God notawiy kukusouwi boro nuhi nabur.
10 Nʼchifukwa chake abale anga, funitsitsani kuti mayitanidwe ndi masankhidwe anu akhale otsimikizika. Pakuti ngati muchita zinthu izi, simudzagwa konse.
10 Imih au ofonah baitumatumayah God eafi naatu rubini imaim yuwa kwana’asfofor turobe kwanabow. Iti na’atube kwanasinaf kwa boro men kwanare’emih.
11 Mudzalandiridwa bwino kwambiri mu ufumu wosatha wa Ambuye ndi Mpulumutsi wathu Yesu Khristu.
11 Basit ef nati na’atube kwanasisinaf kwa boro ata Regah Jesu Keriso ata baiyawasenayan boro baibasit anababatun nit, ma’ama wanatowan ana aiwob kwanarun.
12 Tsono ine ndidzakukumbutsani nthawi zonse za zinthu zimenezi, ngakhale kuti mumazidziwa ndipo kuti munakhazikika mʼchoonadi chimene muli nacho tsopano.
12 Iti ao i an gagamin, isan imih ayu boro matanfufur nuhi anakusisib kwananot. Baise kwa i marasika kwaso’obaka naatu God ana tur kwanowar kwabitumatum i turobe.
13 Ndikuganiza kuti nʼkoyenera ndikanali mu msasa uno, kuti ndikutsitsimutseni ndi kukukumbutsani,
13 Iti i gewasin maiyow ayu yawasu ama’amamaim a not matanfufur akukusisib kwananot nati boun ao isan.
14 chifukwa ndikudziwa kuti posachedwapa ndikuchoka mu msasa uno, monga Ambuye athu Yesu Khristu anandidziwitsiratu.
14 Ayu anotanot iti na’atube i ef gewasin, anayabin Jesu Keriso ata Regah bebeyanamaim au tur eowen ayu boro kafa’imo anamorob.
15 Ndipo ndidzayesetsa kuti nditachoka, mudzakumbukire nthawi zonse.
15 Imih anasinaftobon koufair anit, saise ayu anamomorob ufunamaim iti sawar a notamaim hinama men nuhi hinaburumih.
16 Ife sitinatsate nkhani zongopeka titakuwuzani za mphamvu zake ndi zakubweranso kwa Ambuye athu Yesu Khristu, koma tinaona ndi maso athu za ukulu wake.
16 Kwa au’uwi kwanowar, ata Regah Jesu Keriso ana fair auman boro namatabir maiye nan tafaramaim. I ana fair aki aso’ob, anayabin men sabuw hai baifuwenamaim hibinanakwar anowar a’o’omih. Baise aki taiyuwi mataiyan ana fair gagamin a’i’itin i kwa a tur a’o’owen.
17 Pakuti Iye analandira ulemu ndi ulemerero kuchokera kwa Mulungu Atate atamufikira mawu ochokera ku ulemerero wa ukulu akuti, “Uyu ndi mwana wanga amene Ine ndimukonda, amene ndimakondwera naye kwambiri.”
17 Anayabin aki nati’imaim, God i Tamah naatu ana bonamanamarin auman Jesu Keriso ifai bobora’ara’ah naatu marane fanan Jesu isan eo, “Iti orot i Ayu Natu au yabow, i isan Ayu abiyasisir gagamin maiyow.”
18 Ifeyo tinamva mawuwa akuchokera kumwamba pamene tinali naye pamodzi pa phiri lopatulika lija.
18 Aki Jesu Keriso ana bai’ufununayah nai tounu bairi nati oyaw kakafiyin tafanamaim abat, God isan marane eafare eo aki taiyuwi tainiyan anowar.
19 Tsono ifenso tili ndi mawu a uneneri amene ndi odalirika kwambiri ndipo inu mudzachita bwino mukawasamalira mawuwa, monga kuwunika kumene kukuwala mu mdima, mpaka tsiku lidzayambe kucha, pamene nthanda idzayambe kuwala mʼmitima mwanu.
19 Anayabin aki God fanan anowar, dinab sabuw Keriso isan hio i turobe. Kwa kwanabow gewas fanah kwanab anayabin i kwa a hinow na’atube emamarakaw naatu a Maragias ana marakaw na’atube dogor wanawanan ekukusisiar.
20 Kuposa zonse, inu muyenera kuzindikira kuti palibe mawu a uneneri amene amatanthauzidwa pa okha.
20 Nati i an gagamin kwanaso’ob gewas. Dinab iyab God ana tur Bukamaim hikikirum i men hai notamaim hikirumamih.
21 Pakuti mawu a uneneri sanadze mwa kufuna kwa anthu, koma anthu anayankhula zochokera kwa Mulungu, Mzimu Woyera atawayankhulitsa.
21 Naatu men kafa’imo orot babin ta uwih hikirumamih. Aiyabin! Baise iyab God rurubiniyih i God ana tur hikirum Anun Kakafiyih u’uwih na’atube.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Pedro 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.