2 Coríntios 9
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Nʼkosafunika kuti ndikulembereni za utumiki othandiza anthu a Mulungu.
1 God ana sabuw tafaram Judea tema’am isah siwar kwayai kwabiyafar isan, aisim a fef anakirum a tur ana’owen.
2 Popeza ndikudziwa mtima wanu wofuna kuthandiza, ndipo ndakhala ndikuwawuza monyadira a ku Makedoniya za chimenechi. Ndimawawuza kuti inu a ku Akaya munakonzeka kale chaka chatha kuti mupereke. Ndipo changu chanu chapatsa chidwi ambiri mwa iwo kuti nawonso achitepo kanthu.
2 Anayabin ayu aso’ob kwa Akaiya sabuw a baibais isan mar etei biya emimisir. Masedonia baitumatumayah i ufut kwamur hibogaigiwas hibusuruf teyai’iyi, iti na’atube ao hinonowar anamaramaim sabuw moumurihika yah viri iwa’an hiyai.
3 Koma ndikutumiza abalewo kuti kukunyadirani kwathu pa zimenezi kutsimikizike kuti si kwachabe ndi kuti mukhale okonzeka monga ndinanenera.
3 Baise ata ofonah nah tounu kwa isa aiyunih tenan, anayabin ayu men akokok ai baifa’en kwa isa yabin en namatar. Ana maramaim ayu anan kwa biya anatitit, ayu akokok nati siwar i kwanayabuna na’inu’in anatit. Saise ayu au tur Masedonia isah ao’o niturobe.
4 Pakuti nditabwera kumeneko ndi abale ena a ku Makedoniya, ndikukupezani kuti simunakonzeke, tingadzachite manyazi chifukwa chokudalirani. Koma amene angadzachite manyazi kwambiri ndi inuyo.
4 Asir ayu Masedonia sabuw bairi ananan na’at, kwa siwar men kwayabuna kwama’am it boro biyat na’ohow, anayabin kwa abifai men matar.
5 Choncho ndinaganiza kuti nʼkofunika kupempha abale kuti adzakuchezereni ineyo ndisanafike, ndikuti adzatsirize kukonzekera mphatso zomwe munalonjeza kupereka mowolowamanja. Motero mphatsoyo idzakhala yokonzeratu, ndipo idzakhala mphatso yoperekedwa mowolowamanja, osati mokakamizidwa.
5 Isan imih ayu anotanot tuwatanah orot nah tounu boro ana’uwih au nou hini’iyon hinan hinibaisi kwanayabuna siwar o’on isan, sinafumih kwa’omatan na’atube. Imaibo ayu anan biya ana titit kwa siwar i kwa’o’on kwayabuna sawar kwama’am. Naatu sabuw boro hinaso’ob kwa siwar yai’in isan i dogor tutufin etei kwaitin kwayai men sabuw hi’ukikini kwaya’imih.
6 Takumbukirani mawu awa: Amene adzala pangʼono, adzakololanso pangʼono, ndipo amene adzala zochuluka, adzakololanso zochuluka.
6 Iti tur a notamaim nama. Orot yait masaw teten ebob boro momurih nafour naatu orot yait masaw kukuf ebob boro kikimin nafour.
7 Munthu aliyense apereke chimene watsimikiza mu mtima mwake kuti apereka, osati monyinyirika kapena mokakamizidwa, pakuti Mulungu amakonda wopereka mokondwera.
7 Orot babin ana notamaim bai’ab
8 Ndipo Mulungu akhoza kukudalitsani kwambiri, kuti inuyo nthawi zonse mukhale ndi zinthu zokukwanirani, ndiponso ndi zina zochuluka kuti muthandize pa ntchito zonse zabwino.
8 Naatu o abistan kukokok God i boro nit baise gagaminaka nakarsuwei nit. Saise mar etei o isa sawar etei i nakaram inama naatu o aur i ra’at kwanekwan, imih o karam bowabow gewasih boro inabow.
9 Paja analemba kuti,
9 Na’atube Buk Atamaninamaim eo,
10 Tsono Mulungu amene amapereka mbewu kwa wofesa, ndiponso chakudya kuti adye, adzaperekanso mbewu mʼnkhokwe zanu ndi kuzichulukitsa. Iye adzachulukitsanso zipatso za chilungamo chanu.
10 God mar etei masaw bowayan ub ebitin naatu bay ebitin imih i karam ub kukokok boro nit. Naatu niwa’an hinakubounih hinayen naatu o akaifen gewasinamaim boro moumurihika inafour.
11 Adzakulemeretsani pa zonse kuti mukhale owolowamanja pa nthawi zonse. Ndipo kuwolowamanja kwanu kudzera mwa ife, kudzakhala kuthokoza kwa Mulungu.
11 God boro mar etei o isa nasinaf aur sawar nakaram, saise sabuw moumurin na’in boro inibaisih. Isan imih sabuw moumurin God boro ana merar hinay, anayabin kwa a siwar kwaiyafar in hibaib isan.
12 Ntchito imene mukugwirayi siyongothandiza kokha anthu a Mulungu kupeza zosowa, komanso ikuthandiza kuti anthu ambiri ayamike Mulungu.
12 Bowabow iti na’atube kwasisinaf i men God ana sabuw akisih kwabibaisihimih, baise sabuw afa auman kwabibaisih imih sabuw moumurih maiyow God ana merar teyiy.
13 Chifukwa cha ntchito imene mwawatsimikizira nokha, anthu ena onse adzayamika Mulungu chifukwa cha kumvera kwanu kumene kumaonekera pamene mukuvomereza Uthenga Wabwino wa Khristu, ndiponso chifukwa chowagawira mowolowamanja iwowo pamodzi ndi wina aliyense.
13 Anayabin iti bowabow kwa taiyuw kwa’itin kwaso’ob sabuw boro God hinifai. Anayabin kwa bowabowamaim boro niturobe kwa kwabitumatum naatu nati’imaim sabuw moumurin maiyow hina’itin, God ana merar hinay. Anayabin Keriso ana Tur Gewasin isan kwabosiyasiyar kwao kwabibinan. Naatu dogoroh tutufin etei kwafafarambonen. Naatu sabuw afa bairi kwafafaram etei kwao kwaibasit siwar kwayai, naatu sabuw etei auman. God ana merar hinay,
14 Ndipo iwowo adzakupemphererani mwachikondi chifukwa cha chisomo choposa chimene Ambuye wakupatsani.
14 naatu hai yoyoban o isa i dogoroh wanawananika tit enan, anayabin God ana baigegewasin iwanasum kuma’am.
15 Tiyamike Mulungu chifukwa cha mphatso zake zosaneneka!
15 God ana merar tanay i ana siwar isan tanao tanan men karam.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 9, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.