2 Coríntios 8
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndipo tsopano, abale, tikufuna kuti mudziwe za chisomo chimene Mulungu wapereka ku mipingo ya ku Makedoniya.
1 Taitu tuwai’inah, God ana manaw ana kabeber Kirisiyan sabuw tafaram Masedonia tema’am bi’obaiyih isan i a tur ao’owen kwanaso’ob.
2 Pakati pa mayesero owawitsa, chimwemwe chawo chosefukira ndi umphawi wawo otheratu, anapereka mowolowamanja kwambiri.
2 I yababan kakafih ana routobon wanawanan hirun hin, aurih sawar en baise i hai yasisir i ra’at kwanekwan kabay hiyai.
3 Motero ndikuchitira umboni kuti anapereka mmene akanathera, ndipo mwinanso kuposera mmene akathera kupereka. Anapereka mosakakamizidwa,
3 Ayu a tur ao’owen, abisa hiya’iyai i doroh ana naniyan naatu kokomaim hiyai, baise kabay hiya’iy i tetebon.
4 ndipo anatipempha motiwumiriza kuti tiwapatse mwayi woti nawonso athandize anthu oyera mtima a ku Yudeya.
4 Aki hifefeyani men kikiminta atibaisih kabay turin atayai. God ana sabuw Judea tema’am isah.
5 Iwo anachita moposera mmene ife timayembekezera. Choyamba anadzipereka kwa Ambuye ndipo kenaka kwa ife monga mwa chifuniro cha Mulungu.
5 Abisa hiya’iyai i men aki anot na’atube hitayai, baise gagaminaka hiyai! Wan i hai yawas Regah isan hiya’asair, imaibo God ana kokomaim na’atube hisinaf, hai yawas aki isai hiya’asair hibaisi.
6 Choncho tinamupempha Tito kuti atsirize poti nʼkuti atayamba kale ntchito yachisomoyi pakati panu.
6 Imih Titus aifefeyan, iti bowabow i busuruf na’atuka nabow nan naatu kwa nibaisi iti yabow ana bowabow nabow nisawar.
7 Popeza pa zinthu zonse munachita bwino, monga pachikhulupiriro, poyankhula, pachidziwitso, pakhama lambiri ndi pachikondi chanu pa ife, onetsetsani kuti muchitenso bwino pachisomo ichi chopereka.
7 Baise bowabow tutufin etei kwa isa i karam. Kwa kwabitumitum, kwa a turamaim, kwa a ukwar rerekabamaim. Isan imih aki akokok kwanibaisi bairit yabow ana bowabow tanabow
8 Sindikukulamulirani, koma ndikufuna kuona ngati chikondi chanu nʼchoona pofananitsa ndi changu cha anthu ena.
8 Ayu men roufafar ta aya’iy. Baise mi’itube sabuw ani’obaiyih hai naniyan kabay ya’inamaim nama saise kabay hinayai Kirisiyan sabuw afa hinibaisih, ayu asisinaftobon ana so’ob gewas kwa a yabow i turobe.
9 Pakuti mukudziwa chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu, kuti ngakhale anali wolemera, koma chifukwa cha inuyo anasanduka wosauka, kuti umphawi wakewo, inuyo mulemere.
9 Kwa ata Regah Jesu Keriso ana manaw ana kabeber i kwaso’ob. I isan sawar etei karam, baise kwa isa na akir orot matar saise i ana bai’akiramaim kwa boro niwa’ani kwanan totobuyoy wairaf kwanamatar.
10 Ndipo nawa malangizo anga pa zoyenera inu kuchita pa nkhaniyi. Chaka chatha munali oyamba, osati ongofuna kupereka kokha komanso okhala ndi mtima ofuna kupereka.
10 Ayu au not i iti na’atube anotanot, kwa iyab iti bowabow fai komur kwabusuruf kwabowabow ana gewasin boun kwanisawaren. Kwa baitinin ana bowabow i wan kwabusuruf kwabow, men bowabow sinaf akisin. Baise takokok tanasinaf namatar.
11 Tsopano tsirizani ntchitoyi, ndipo changu chanu chofunitsitsa kugwira ntchitoyi ndi kuyitsiriza chichitike molingana ndi zimene muli nazo.
11 Iti bowabow kwabusuruf kwabowabow i kwanisawar, saise abistan kwakok sinaf isan kwa yayakitifuw i kwanasinaf namatar naatu abistan kwa aur ema’am i kwanayai.
12 Ndipo ngati mtima ofunitsitsa ulipo, mphatsoyo imalandiridwa molingana ndi zimene munthuyo ali nazo, osati zimene alibe.
12 A naniyanamaim baitinin nama’am, o a siwar i God ebaib anayabin i aurin sawar karam, abistan i aurin sawar men kakaram i men abistan ta.
13 Cholinga chathu sikuti tipeputse ena pamene inuyo mukuvutika, koma kuti pakhale kufanana.
13 Aki men akokok afa isah aniwa’an naham naatu kwa isa aniwa’an nafokar, baise akokok roun roun na’abara’ah kwanibaibaisbonen.
14 Zambiri zimene muli nazo pakati panu muthandize nazo osowa, kuti nawonso akadzakhala nazo zambiri adzakuthandizeni pa zosowa zanu. Cholinga nʼkuchita mofanana,
14 Iti boun ana veya, kwa a mouramaim abistan hai kokok kwanibaisih, saise i hai mour ana veya kwa abistan kwakokok boro hinibaisi. Naatu nati kwa bairi wan kwayi anafofonin.
15 monga kwalembedwa kuti, “Iye amene anatola zambiri sizinamutsalireko ndipo amene anatola pangʼono sizinamuchepere.”
15 God ana tur Buk Atamaninamaim hikirum inu’in, “Naatu orot babin yait masaw teten ebob naatu orot babin yait masaw kukuf ebob i hairi anafofonin tefafour.”
16 Tithokoze Mulungu amene anayika mu mtima wa Tito changu chomwecho chimene ine ndili nacho pa inu.
16 Ayu God ana merar ayiy! Iti not ta’imon ayu anotanotabe Titus kwa isa enotanot.
17 Pakuti Tito sanangovomera kokha pempho lathu, koma yekha anafunitsitsa kwambiri kubwera kwa inu mwa iye yekha.
17 Anayabin aki Titus i men abifefeyan akisin fanai bai enanamih, baise i taiyuwin ana kokomaim auman kwa nibaisimih enan.
18 Ndipo tikumutumiza pamodzi ndi mʼbale amene mipingo yonse yamuyamikira chifukwa cha utumiki wake wa Uthenga Wabwino.
18 Naatu aki ai of ta i aiyun hairi tenan, ekaleisia sabuw etei i wabin tebobora’ah, anayabin tur gewasin eo ebibinan isan.
19 Chowonjezera china nʼchakuti anasankhidwa ndi mipingo kuti atiperekeze pamene ife tikukapereka zopereka, zimene tikuchita pofuna kupereka ulemu kwa Ambuye mwini ndi kuonetsa kufunitsitsa kwathu pothandiza.
19 Aki iti bowabow asisinaf, baise bowabow ta auman ekaleisia sabuw hirubin aki bairi anan nibaisi yabow ana bowabow anabow isan. Iti bowabow isan i Regah wabin abora’ara’ah, naatu sinafumaim abi’obaiyih.
20 Tikufuna kupewa kutikayikira kulikonse za mmene tikuyendetsera mphatso zochulukazi.
20 Aki a siwar kwaya’iy akakaif gewasin men aniwa’an kakaf orot babin isai tur hina’omih.
21 Pakuti tikuyesetsa kuchita zolondola, osati pamaso pa Ambuye pokha komanso pamaso pa anthu.
21 Anayabin aki bowabow i mutufurin gewasin anabow isan i akokok, men Regah matanamaim akisin, baise sabuw matahimaim auman.
22 Kuwonjezera apo, tikuwatumiza pamodzi ndi mʼbale wathu, amene nthawi zambiri watitsimikizira mʼnjira zosiyanasiyana kuti ndi wachangu ndiponso chifukwa ali ndi chikhulupiriro chachikulu mwa inu.
22 Isan imih aki ata of tabo arubin bairi tenan, mar moumurin maiyow ef afa’ane arutubun a’itin i ebi’o’orot, i ekokok kwanekwan kwa nibaisih, anayabin kwa tafamaim i fair ebaib.
23 Kunena za Tito, ndiye mnzanga ndi wogwira naye ntchito pakati panu. Kunena za abale athu, ndiwo oyimirira mipingo ndi olemekezetsa Khristu.
23 Titus i ayu au of naatu ayu bowturou, ayu airi kwa anibaisi anabow, boun it tuwat na’atube. Iti orot rou’ab i ekalesia hirubin naatu Keriso wabin isan i tebobora’ara’ah.
24 Choncho anthu amenewa atsimikizireni za chikondi chanu ndipo adziwe chifukwa chimene ife timakunyadirani, kuti mipingo yonse iwone chimenechi.
24 Isan imih a yabow kwani’inuw iti oro’orot hina’itin saise ekaleisia hinasu’ubih gewas naatu hinaso’ob aki gewasinawat asisinaf imih kwa isa ao abi’o’orot.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 8, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.