2 Coríntios 7
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Abwenzi okondedwa, popeza tili ndi malonjezo amenewa, tiyeni tidziyeretse, kusiyana nazo zilizonse zimene zikhoza kudetsa thupi ndi mzimu, ndipo tiyesetse kukhala oyera mtima poopa Mulungu.
1 Are teitu tuwai’inah iti omatanen i’ubaiyit eo tanowar. Imih it abistanamaim iwa’an biyat naatu ayubit kato emamatar i tanakusouwen, biyat ni’uhew kakafiyin namatar God tanabiruw tanama.
2 Mutipatse malo mʼmitima mwanu. Ife sitinalakwire munthu aliyense, kapena kuyipitsa munthu aliyense, kapena kumuchenjerera munthu aliyense.
2 Dogor kwanabotawiy ereyasisir kwanabuwi anayabin aki men yait ta kakafin isan asinaf, aki men yait ta agurus, aki men yait ta ai a’afiy.
3 Sindikunena izi kuti mupezeke olakwa. Ndinanena kale kuti ife timakuganizirani kwambiri kotero kuti tili pamodzi, ngakhale tikhale moyo kapena timwalire.
3 Ayu iti tur ao’o i men kwa akukusairimih. Anayabin ayu marasika ao kwanowaraka, kwa aki dogorei’imaim kwama’am mar etei, bairit yawasit tanama ai tanamorob.
4 Ndimakukhulupirirani kwambiri ndipo ndimakunyadirani kwambiri. Ndikulimbikitsidwa kwambiri; mʼmasautso athu onse, chimwemwe changa chilibe malire.
4 Ayu kwa tafamaim fair gagamin maiyow abaib, imih ayu abi’o’orot men kafaita. Anayabin yare wanawanah arur ayu koufair gagamin maiyow abaib, ayu mar etei yasisir dogorou awan karatan ekakarsuwei.
5 Pakuti titafika ku Makedoniya, sitinapume nʼkomwe, koma tinavutitsidwa mbali zonse. Kunja kunali mikangano, ndipo mʼmitima mwathu munali mantha.
5 Aki ana tafaram Masedonia atitit ana veya, aki men aiyarir. Nati’imaim yare ef ta ta’ane himatar, sabuw taiyuwih nane hibigamigam wanawanah arun naatu aki dogorei wanawanan erebirubir ama.
6 Koma Mulungu, amene amatonthoza mtima wopsinjika, anatitonthoza mtima ndi kufika kwa Tito,
6 Baise sabuw iyab hai not erara’iy God koufair ebitih, imih Titus nan i ata koufair ta bai na itit.
7 sikubwera kwake kokhako, komanso mawu achilimbikitso amene analandira kuchokera kwa inu. Iye anatiwuza kuti mukufuna kundiona, zachisoni chanu chachikulu, ndi kudzipereka kwanu kwa ine, motero chimwemwe changa chinachuluka kuposa kale.
7 Naatu men i ana bainanawan akisin baise kwa auman koufair kwaitin. Mi’itube yababan gagamin maiyow ayu isou kwabaib aki ai tur eowen anowar, kwa dogor babanaika kwabiyababan, kwa a not gagamin maiyow ayu isou, isan imih ayu au yasisir i ra’at kwanekwan.
8 Ngakhale kalata yanga ija inakupwetekani mtima, sindikudandaula kuti ndinalemberanji. Ngakhale zinandikhudza, ndikudziwa kuti kalata yanga inakupwetekani, koma kwa kanthawi kochepa.
8 Imih ayu au fefemaim yababan anabit na’at, ayu men abiyababan. Baise iti fef akikirum i kwa rabi, nati boro mar kikimin kwaniyababan.
9 Koma tsopano ndine wokondwa, osati chifukwa chakuti kalatayo inakupwetekani, koma chifukwa chakuti chisoni chanu chinakuthandizani kutembenuka mtima. Pakuti munamva chisoni monga mmene Mulungu amafunira, choncho simunapwetekedwe mwanjira iliyonse.
9 Baise boun i ayu abiyasisir men kwa kwabiyababan isan, baise anayabin kwa a yababan bonawiyi dogor kwaikitabir. Nati yababan i God notanotabe matar, naatu imih men ef ta ema’am kwa ani’afiyi.
10 Chisoni chimene Mulungu amafuna chimabweretsa kutembenuka mtima komwe kumabweretsa chipulumutso, ndipo sichikhumudwitsa. Koma chisoni cha dziko lapansi chimabweretsa imfa.
10 Anayabin God kwanabiyababan iti na’atube temamataramaim boro nibaisi nabonawiyi yawas kwanab baise orot babin tafaram ana yawasamaim tema’am boro morob kwanatita’ur.
11 Taonani zimene chisoni chimene Mulungu amafuna chatulutsa mwa inu. Chatulutsa khama lalikulu, chakuthandizani kuti mudzikonze nokha, chakukwiyitsani kwambiri, komanso chakupatsani mantha aakulu. Chakuchititsani kuti mufune kundiona ine, mwakhudzidwa kwambiri ndipo mukufuna kuonetsetsa kuti chilungamo chachitikadi. Pa nkhani yonseyi, mwaonetsadi kuti ndinu osalakwa.
11 Kwa a yababanamaim God ro’oro’on kwa wanawanane titit kwai’itin. Bowabow gewasin turobe’emaim kwasisinaf, kakafih men kwakokok, bora’atamaim kwama’am, kwanunu’afe’af ayu itu isan, ayu wasfafaru isan kwanotanot, ma gewas isan kwakokok. Kwa asinafumaim ebiturobe kwa a kakafin ta en.
12 Choncho ngakhale ndinakulemberani kalata ija, sindinayilembe ndi chifukwa cha amene analakwayo kapena wolakwiridwa, koma ndinayilemba kuti inuyo muone kudzipereka kwanu kwa ife pamaso a Mulungu.
12 Ayu fef iti akikirum i men yait ta kakafin sisinaf isan, o men yait ta isa kakafin sisinaf isanamih. Baise ayu iti fef akikirum anayabin God nanamaim kwa anababatun aki isai i kwanotanot gagamin maiyow.
13 Zimenezi zatilimbikitsa kwambiri.
13 Ana an nati isan aki koufair abai. Imaim aki ai koufair tafan ya’abar, Titus biyasisir a’i’itin aki akawasa men kikimin ta, anayabin i ayubinane kwa etei’imak a naniyan bora’ah.
14 Ndinamuwuza kuti ndimakunyadirani, ndipo simunandichititse manyazi. Koma monga zonse zimene tinakuwuzani zinali zoona, tsono zomwe ndinawuza Tito zokunyadirani zinali zoona.
14 Titus matanamaim ayu kwa aifai, naatu kwa ayu men kwaibiya’uhuwu’umih, kwa isa aki anababatunamaim ao, aki aibaifa’en Titus itin i turobe.
15 Ndipo chikondi chake pa inu nʼchachikulu kwambiri akakumbukira kuti nonse munali omvera, munamulandira ndi mantha ndi kunjenjemera.
15 Isan imih Titus ana yabow kwa isa i ra’at kwanekwan. I ana notamaim kwa mi’itube kwabogaigiwas naatu mi’itube kwabir a uma hi’oror auman ana merar kwayi kwabaib, ana tur anonowar isan.
16 Ndine wokondwa kuti ndingathe kukukhulupirirani pa zonse.
16 Ayu abiyasisir gagamin maiyow bounabo nuhunafot kwa tafamaim fair anab anabatkikin.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 7, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.