2 Coríntios 2
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Kotero ndinatsimikiza maganizo anga kuti ndisachitenso ulendo wina owawa wobwera kwanuko.
1 Imih ayu au not ayai sawar uf men anan aninanawani yababan ta ibanak anit maiye.
2 Pakuti ngati ndikumvetsani chisoni, kodi angandisangalatse ndani, kupatula inuyo amene ndakumvetsani chisoni?
2 Ayu kwa ana’uw kwanikwaniy yababan anabit na’at, yait boro yasisir ayu nitu?
3 Nʼchifukwa chake ndinakulemberani monga ndinachitiramo kuti nditabwera kwanuko ndisadzamve chisoni ndi anthu oyenera kundisangalatsa. Ndinali ndi chikhulupiriro ndi inu nonse kuti inuyo mukakhala ndi chimwemwe poona kuti inenso ndili ndi chimwemwe.
3 Ana’an iti isan ayu afef akikirum saise ayu anan na’at kwa bai yasisiru’umih kwatasisinaf i men tiyababanu. Ayu aitutumi kwa etei isa, ayu au yasisir kwa boro bairit taniyasisir.
4 Pakuti ndinakulemberani kalata ija ndili wopsinjika ndi wowawidwa mtima kwambiri ndi kutuluka misozi yambiri, osati pofuna kukumvetsani chisoni koma kuti ndikudziwitseni kuti ndimakukondani kwambiri.
4 Anayabin ayu dogorou babanika yababan kufutu naatu erererey auman a fef akirum, men kwa baiyababani isan, baise ti’obaiyi ayu kwa isa i dogorou babanika abiyabuwi.
5 Koma ngati wina wamvetsa chisoni, sanamvetse chisoni ine ndekha, koma koposa mosawonjezera wakhumudwitsa nonsenu, kunenatu mosawonjezera.
5 Yait ta yababan nasisinaf na’at, men ayu akisu ebiyababanu’umih, baise kwa tutufin etei ebiyababani, ibanak men kwana’itin gagaminamih.
6 Chilango chimene ambiri a inu mwamupatsa munthu ameneyu nʼchokwanira.
6 Sabuw tutufin etei hio hibasit orot babin baimakiy ebaib nati anafofonin.
7 Mʼmalo mwake tsono, muyenera kumukhululukira ndi kumulimbikitsa mtima kuti asamve chisoni choposa muyeso, angataye mtima.
7 Baise gewasin ana kakafin kwananotawiy naatu koufair kwanitin, saise i boro men yababan niwanasum.
8 Choncho ndikukupemphani kuti mutsimikizire chikondi chanu pa iye.
8 Isan imih kwa abifefeyani, kwanau gewas naso’ob, kwa i kwabiyabuw.
9 Cholinga china chimene ndinakulemberani kalata ija chinali chofuna kukuonani ngati mudzandimvera pa zonse.
9 Ayu iti fef akikirum i akokok ataso’ob gewas, karam routobon kwatisnowaten naatu bai’obaiyen etei kwatifanabow.
10 Aliyense amene mumukhululukire, inenso ndimukhululukira. Ndipo ndikakhululukira, ngati pali kanthu koti ndikhululukire, ndiye kuti ndakhululuka chifukwa cha inu pamaso pa Khristu,
10 Kwa orot babin ta ana kakafin kwananonotawiy na’at, ayu auman i anotanotawiy, abisa anonotawiy ana kakafin ta nama’am na’at, i Keriso nanamaim kwa wab isan anotawiy,
11 kupewa kuti Satana angapezere mpata pa ife, pajatu timadziwa machenjerero ake.
11 saise Satan men karam nikubibiruwit, anayabin it taso’ob i ana yakitifuwen.
12 Tsono nditafika ku Trowa kuti ndilalikire Uthenga Wabwino wa Khristu, nʼkupeza kuti Ambuye anditsekulira khomo,
12 Ayu Keriso ana tur gewasin binan isan ana Troas atit naatu Regah au ef botawiy nati’imaim ata binan isan.
13 ndinasowa mtendere mu mtima mwanga, chifukwa sindinapezeko mʼbale wanga Tito. Choncho ndinatsanzikana ndi anthu kumeneko nʼkupita ku Makedoniya.
13 Baise ayu yababan abai, anayabin ayu teu Titus men atita’ur. Imih sabuw nati’imaim hima’am aotuturih naatu an Masedonia.
14 Koma tithokoze Mulungu amene amatitsogolera nthawi zonse monga ogwidwa ku nkhondo a Khristu pa chipambano chake. Tsono amatigwiritsa ntchito yofalitsa ponseponse nzeru zodziwira Khristu ngati fungo labwino.
14 Baise God ana merar tanay! Anayabin mar etei i nawiyit Keriso ana baigegsairen isan irar yoman tatatain naatu itane God tasu’ub. boun ai ebuwayan yamurin mamarin etasasar etitit na’atube.
15 Pakuti kwa Mulungu ndife fungo labwino la Khristu pakati pa iwo amene akupulumutsidwa ndi amene akuwonongeka.
15 Anayabin it i Keriso ana yamurin mamarin gewasin, God isan sibor eya’iy, nati sabuw iyab yawas hibaib naatu iyab temomorob isah.
16 Kwa amene akuwonongeka ndife fungo la imfa, limawapha. Ndipo kwa amene akupulumuka ndife fungo lamoyo, limawapatsa moyo. Ndani angayithe ntchito yotereyi?
16 Sabuw iyab tekakasiy i sabuw himorobobe biyah mas yamurin kakafin, baise sabuw iyab yawas hibaib i yawas anayamurin mamarin. Iti bowabow isan yeit i karam nabow?
17 Kusiyana ndi ena ambiri, ife sitilalikira Mawu a Mulungu kuti tipeza phindu. Mʼmalo mwake, ife mwa Khristu timayankhula pamaso pa Mulungu moona mtima, monga anthu otumidwa ndi Mulungu.
17 It men sabuw tutufin etei tesisinafube’emih naatu men God ana tur tabai sawar gidigidih na’atube efamaim tatobon tareremor na’atube’emih. Baise God iyunit Keriso ana bowayah tamatar, God nanamaim turobe tabibinan.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.