2 Coríntios 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu, pamodzi ndi mʼbale wathu Timoteyo,
1 Ayu Paul God ana kokomaim Keriso Jesu ana turabarayan amatar naatu it turat Timothy airi kwa ekalesia sabuw tafaram Corinth kwama’am naatu God ana sabuw etei tafaram Akaiya wanawanan kwama’am isa fef akirum abiyafar.
2 Mukhale ndi chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu.
2 Ayoyoban God it Tamat naatu Regah Jesu Keriso’one manaw kabeber naatu tufuw kwa etei isa nama.
3 Alemekezeke Mulungu, Atate a Ambuye athu Yesu Khristu, Atate achifundo chonse, Mulungu wachitonthozo chonse.
3 God it Tamat naatu ata Regah Jesu Keriso Tamah, ana merar tanay anayaabin kabeber ana’an ine enan naatu ata baibais etei ana God.
4 Iye amatitonthoza ife mʼmavuto athu onse, kuti ifenso tithe kutonthoza amene ali pavuto lililonse ndi chitonthozo chimene ife tilandira kwa Mulungu.
4 Ata yare moumurih na’in wanawanah tarur i koufair koubainunub ebitit, imih nati koufair koubainunub ta’imon God it bitit, karam sabuw iyab yare koun hiyen tere’er koufair koubainunub tanitih.
5 Pakuti monga momwe tili mʼmasautso pamodzi ndi Khristu, momwemonso Khristu amatitonthoza kwambiri.
5 Anayabin Keriso ana bai’akir bairi tafafaram na’atube God ana koufair Keriso wanawananamaim ata koufair boro gagamin na’in nakarsuwei nare tanab.
6 Ngati ife tikusautsidwa, nʼchifukwa choti inu mutonthozedwe ndi kupulumutsidwa. Ngati ife tikutonthozedwa nʼchifukwa choti inu mutonthozedwe, ndi chitonthozo chimene chimabweretsa mwa inu kupirira kosawiringula pa zosautsa zomwe timasauka nazo ife.
6 Aki abi’akir i kwa a koufair naatu a yawas bain isan. Aki koufair abaib kwa auman boro koufair kwanab yate nanub nawainabi a yawas kwanab. Nati bai’akir ta’imon aki na’atube wanawanan arun asora’ub.
7 Ndipo chiyembekezo chathu pa inu nʼcholimba chifukwa tikudziwa kuti monga momwe mumamva zowawa pamodzi nafe, momwemonso mumatonthozedwa nafe pamodzi.
7 Imih kwa isa aki nuhifot ama’am, anayabin Keriso ana bai’akir turin kwabaib isan boro God ana koufair nit Keriso wanawananamaim.
8 Abale, sitikufuna kuti mukhale osadziwa za masautso amene tinakumana nawo mʼchigawo cha Asiya. Tinapanikizidwa koopsa kuposa muyeso woti nʼkutha kupirira, mwakuti sitinkadziwa kuti nʼkukhalabe ndi moyo.
8 Taitu tuwai’inah aki akokok kwanaso’ob tafaram Asia wanawanan aki hai fokarih kakafih wanawanan arun bai’akir gagamin maiyow abai anot i boro ata morob.
9 Zoonadi, tinamva mʼmitima mwathu chilango cha imfa. Koma izi zimachitika kuti tisangodzidalira mwa ife tokha koma Mulungu yemwe amaukitsa akufa.
9 Turobe, aki naniyi atatam i morob isan hirubin. Baise iti namamatar i ebi’obaiyit it men taiyuwit tanitutumit, baise God tanitumitum i akisinamo murumurubih ebimisuruwih.
10 Mulungu watilanditsa ku zoopsa zotere za imfa, ndipo adzatilanditsanso. Ife tayika chiyembekezo chathu pa Iyeyo kuti adzapitiriza kutilanditsabe.
10 Morob kakafin wan ayenabo botaiti atit, naatu boro nabotaiti anatit maiye. I tafanamaim aki ai nuhifot i boro na’atuka nabotaititi anatit.
11 Mutithandize potipempherera. Pamenepo ambiri adzathokoza mʼmalo mwathu, chifukwa cha chisomo chake poyankha mapemphero a anthu ambiri.
11 Na’atube kwa a yoyobanamaim aki kwanibaisi. Saise God boro a yoyoban niya’afuten naatu aki nigegewasini, naatu sabuw moumurin maiyow God boro ana merar hinay aki bigegewasini isan.
12 Tsono chonyadira chathu nʼchakuti, chikumbumtima chathu chimatitsimikizira kuti timakhala bwino mʼdziko lapansi, makamaka pa ubale wathu ndi inu. Takhala moona mtima ndi oyera mtima. Sitinachite chomwechi mwa nzeru ya dziko lapansi koma monga mwa chisomo cha Mulungu.
12 Aki aora’ara’at anayabin iti tafaramaim ama’am ai not iu’uwi aiyawas naatu ai baita’ay kwa bairit i kakafiyin naatu mutuforomaim asisinaf. Aki ai sinaf etei i Godane men tafaram ana ukwar rerekab, baise God ana manaw ana kabeberamaim.
13 Pakuti sitikukulemberani zoti simungawerenge kapena kumvetsetsa.
13 Anayabin aki fef kwa isa akikirum tur etei i mutufor naatu rereb yah karam kwaniyab boro naniyan kwanab.
14 Monga mwamva pangʼono chabe, ndikuyembekeza kuti mudzamvetsa kwenikweni, kuti mutha kutinyadira monga ife tidzakunyadirani, pa tsiku la Ambuye Yesu.
14 Abisa boun akikirum kwanabiyab boro men naniyan kwanab, baise Ata Regah Jesu namatabir nanan ana veya boro kwanaso’ob, aki isai boro kwanaora’ara’at, naatu aki auman boro kwa isa ana’ora’ara’at.
15 Popeza ndinatsimikiza mtima za ichi, nʼchifukwa chake ndinafuna kuti poyamba, ndidzakuchezereni kuti mupindule pawiri.
15 Anayabin iti isan ayu aitumatum, ayu ayakitifuw wan kwa aninanawani saise kwa agewasin boro tafan tanaya’abar.
16 Ndinafuna kuti ndidzakuchezereni pa ulendo wanga wopita ku Makedoniya ndi kudzakuonaninso pochokera ku Makedoniyako kuti inu mudzandithandize pa ulendo wanga wopita ku Yudeya.
16 Ayu akokok ef aumatan au Masedonia ananan anarun ana’iti naatu Masedonia’ane anamamatabir boro anarun ana’iti. Imaibo kwa boro au ef isan kwanibaisu anan Judea.
17 Kodi pamene ndinkakonzekera zimenezi, mukuganiza kuti ndinkachita mwachibwana? Kapena kuti ndinkaganiza ngati mwa dziko lapansi; kuti ndikhoza kumanena kuti, “Inde, Inde,” nthawi yomweyo nʼkumatinso “Ayi, Ayi?”
17 Kwa boro iti na’atube kwanao, namihibe ma yayakitifuw naatu kwahihir ema’am. Kwanotanot ayu orot babin teo tibibasit naatu sinafu’e tema’am i orot ta?
18 Koma zoona monga Mulungu ali wokhulupirika, uthenga wathu kwa inu siwakuti, “Inde” nʼkutinso “Ayi.”
18 God ana tur mar etei turobe eo, imih aki ai tur kwa isa ao i turobe men baifuwen.
19 Pakuti Yesu Khristu mwana wa Mulungu amene ine, Silivano ndi Timoteyo tinamulalikira pakati panu sali “Inde” yemweyonso “Ayi.” Koma nthawi zonse mwa Iye muli “Inde.”
19 Anayabin God Natun Jesu Keriso isan kwa wanawanamaim ayu Silas naatu Timothy abibinan i turobe, men baifuwen.
20 Pakuti ngakhale malonjezo a Mulungu atachuluka chotani, onsewo ndi “Inde” mwa Khristu. Kotero kuti mwa Iye, ife timati “Ameni” kuchitira Mulungu ulemu.
20 God ana’omatanen etei i Keriso wanawananamaim hina hiturobe. I wabin i “Turobe.” Imih i wanawananamaim aki “Amen” a’o God wabin abobora’ara’ah.
21 Tsono ndi Mulungu amene anachititsa kuti inu ndi ife tiyime molimba mwa Khristu. Anatidzoza ife,
21 God akisin sinafit kwa aki bairit yanowahit Keriso wanawananamaim tababatkikin,
22 nayikanso Mzimu wake mʼmitima mwathu kutitsimikizira za mʼtsogolo.
22 I nowanamih ikwahit naatu Anun Kakafiyin dogorotamaim iwan na’atube, i anababahor abistan gewasin boro uf enanan isan.
23 Mulungu ndi mboni yanga kuti sindinabwererenso ku Korinto kuno kuti ndisakumvetseni chisoni.
23 God i ayu au sifroubonenayan na’atube, ayu dogorou wanawanan i so’ob. Ayu akokok kwa aniyaturi imih boro men anamatabir maiye anan Corinth.
24 Sikuti ife tikufuna kukhala olamulira chikhulupiriro chanu, koma timagwira nanu ntchito pamodzi kuti mukhale achimwemwe, chifukwa ndinu okhazikika kwambiri mʼchikhulupiriro.
24 Aki men kwa abaitumatum anunufuruw, baise bairit tanabow a yasisir isan, anayabin baitumatumamaim kwababatkikin.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.