2 Coríntios 13

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Uwu ndi ulendo wachitatu ndikubwera kudzakuyenderani. “Nkhani itsimikizike ndi umboni wa anthu awiri kapena atatu.”
1 Iti boun i mar baitonin kwa isa aninanawani. Buk Atamaninamaim hikirum hio, “Menamaim tur hibow tetitit sif roubinenayan rou’ab o tounu na’atube sif hinaruboun.”
2 Ndinakuchenjezani kale pamene ndinali nanu ulendo wachiwiri uja. Tsopano ndikubwereza ndisanafike. Ndikabweranso sindidzachitira chifundo amene anachimwa poyamba paja kapena wina aliyense amene anachimwa,
2 Ayu baimatnuwen marasika ao kwanowaraka, mar bairu’abin ana bairit tama’am ana mar. Ayu boun i ef yok ama’am baimatnuwen ibanak tafan ao maiye. Ayu kwa isa anamamatabir sabuw iyab bowabow kakafih hima tisisinaf naatu yait marasika ma sisinaf boro men yait ta baimakiy wan nahaiwamih.
3 popeza mufuna chitsimikizo chakuti Khristu akuyankhula kudzera mwa ine. Iye siwofowoka pofuna kuchita nanu koma ndi wamphamvu pakati panu.
3 Kwa kwakokok kwaniturobe Keriso i aki wanawana’imaim eo’o. Anamaramaim kwa wanawanan narun nabowabow i men ririmin kwana’itin, baise i ana fair i ra’at kwanekwan kwa wanawanamaim.
4 Pofuna kutsimikizira, anapachikidwa ali wofowoka koma ali ndi moyo mwamphamvu ya Mulungu. Chomwechonso, ife ndife ofowoka mwa Iye, koma tidzakhala ndi moyo pamodzi naye ndi mphamvu ya Mulungu, potumikira pakati panu.
4 Anayabin kwa itin so’ob gewas isan, Keriso onaf afe’enamaim ririm, baise God ana fairamaim i yawas ema’am. Aki na’atube, i wanawananamaim ariririm, baise God ana fairamaim aki boro bairi anama kwa isa anabow.
5 Tadzisanthulani nokha kuti muone ngati muli mʼchikhulupiriro; dziyeseni nokha. Kodi simuzindikira kuti Khristu Yesu ali mwa inu, ngati si choncho mwalephera mayesowa?
5 Kwa taiyuw kwananutitiyi naatu kwafufuni kwana’itin, turobe kwa baitumatumamaim kwama’am. Kwa kwaso’ob Keriso Jesu i kwa wanawanamaim ema’am. Men nama’am na’at kwa routobon i kwara’iy anababatun.
6 Ndipo ndikhulupirira kuti mudzazindikira kuti ife sitinalephere mayesowo.
6 Naatu ayu abitumatum kwa boro kwana’inani aki routobon men ara’iyemih.
7 Tsopano tikupemphera kwa Mulungu kuti musadzachite kanthu kena kalikonse kolakwa. Osati chifukwa choti anthu aone kuti ife tapambana mayesowo koma kuti mudzachite zokhoza ngakhale anthu atamationa ngati olephera.
7 Baise God isan ayoyoyoban saise kwa boro men kakafin ta kwanasinaf. Men routobon abai abatabat isan sabuw hina’iti, baise aki akokok abistan gewasin kwanasinaf, aki routobon anarara’iy na’at.
8 Pakuti sitingachite chilichonse chotsutsana ndi choonadi, koma chokhacho chovomerezana ndi choonadi.
8 Anayabin aki men karam Turobe isan anirakit, baise Turobe akisin i isan anabat anabow.
9 Ife timasangalala kuti pamene tafowoka, inu muli amphamvu; ndipo pemphero lathu ndi lakuti mukhale angwiro.
9 Aki ariririm i abiyasisir, baise kwa i kwafafair imih aki auman ayoyoyoban kwa boro mi’itube kwanan kwanigewasin.
10 Nʼchifukwa chake ndimalemba zinthu zoterezi pamene ndili kutali, kuti ndikabwera ndisadzagwiritse ntchito ulamuliro wanga mokalipa, uwu ndi ulamuliro umene Ambuye anandipatsa kuti ndikukuzeni inu osati kukuwonongani.
10 Ayu boro men bairit tanama, iti isan kwa isa fef akirum aiyafar enan, ayu i ef yokaika ama’am, anamaramaim ayu anan kwa biya anatit men fair Regah bitu imaim ana gurusi’imih. Baise Regah fair bitu imaim kwa ana wowabi kwanayen.
11 Potsiriza abale, ndikuti tsalani bwino. Yesetsani kukhala angwiro, mvetsetsani pempho langa, khalani a mtima umodzi, khalani mwamtendere. Ndipo Mulungu wachikondi ndi mtendere adzakhala nanu.
11 Are teitu tuwai’inah, bounabo ao’otuturi kwanama’o! A Gewasin isan kwaitafofor, au fefeyan isan tain kwanarub, turanah bairi kwanifanabow, tufuwamaim kwanama. Naatu tufuw yabow ana God boro bairi kwanama wanatowan.
12 Lonjeranani ndi mpsopsono wachiyero.
12 A ofonah hai merar kwanay kwanabuwih kwanakarmamayih erererey auman.
13 Anthu onse a Mulungu akupereka moni.
13 God ana sabuw etei kwa amerarayow tebiyafar.
14 Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu, ndi chikondi cha Mulungu, ndi chiyanjano cha Mzimu Woyera zikhale ndi inu nonse.
14 Ayu ayoyoyoban, Regah Jesu Keriso ana manaw ana kabeber, naatu God ana yabow, naatu Anun Kakafiyin ana baita’ayomaim bairi kwanama wanatowan.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 13, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.