2 Coríntios 12
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ndiyenera kupitiriza kudzitamandira. Ngakhale palibe choti ndipindule, ndipitiriza kufotokoza za masomphenya ndi mavumbulutso ochokera kwa Ambuye.
1 Ayu boro ana’ora’ara’at. Baise boro men imaim tanab. Ayu anarabon Regah ana i’inan ai’itah naatu abistan hirererereb ai’itah imaim anao kwananowar.
2 Ndikudziwa munthu mwa Khristu amene zaka khumi ndi zinayi zapitazo anatengedwa kupita kumwamba kwachitatu. Sindikudziwa ngati zinachitika ali mʼthupi kapena ayi, zimenezo akudziwa ndi Mulungu.
2 Ayu aso’ob kwamur etei 14 Keriso ana baitumatumayan orot ta bai au mar yen, yatetoro’ot mar ana ruf baitonin wanawanan run. Men taso’ob biyan tutufin yen o ayubin tabaratait yen. Ayu men aso’ob God akisin so’ob.
3 Ndipo ndikumudziwa munthu ameneyu. Sindikudziwa ngati zinachitika mʼthupi kapena ayi, zimenezo akudziwa ndi Mulungu.
3 Ayu aso’ob nati orot, men aso’ob biyan tutufin yen o i anuninawat tabaratait yen. God akisin so’ob.
4 Munthuyu anatengedwa kupita ku paradizo. Ndipo anamva zinthu zosatheka kuneneka, zinthu zimene munthu saloledwa kunena.
4 I yen in Paradise, naatu nati’imaim tur nonowar i ananowarin ta, men karam boro tanao tanakubuna.
5 Ndidzatamanda za munthu ngati ameneyu, koma sindidzadzitamandira ine mwini kupatula za kufowoka kwanga.
5 Imih orot nati na’atube boro isan ana’ora’ara’at, baise men ayu isou ana’ora’ara’at.
6 Ngakhale nditafuna kudzitamandira, sindingakhale chitsiru, chifukwa ndikunena zoona. Koma ndimapewa kuti pasapezeke munthu wondiganizira moposera chimene ndili chifukwa cha zimene ndimachita kapena kuyankhula,
6 Ayu anakok ana’ora’ara’at na’at, men koko’aw kwanarouw kwanao, anayabin ayu turobe ao. Baise boro men ana’ora’ara’at, anayabin ayu abistan ao kwanonowar naatu kwa’i’itin men akokok o yait ta a not yate’eka inanot wabu inabora’ah.
7 kapena chifukwa cha mavumbulutso aakulu kuposa awa. Choncho, kuti ndisadzitukumule, ndinayikidwa minga mʼthupi langa, wamthenga wa Satana, kuti adzindizunza.
7 Ayu men nati ina’inan gewasih God isou iwa’an irerereb ai’itah isah ao’omih. Baise Satan ana tounamatar iyafar na biyou kokoramaim yi bai’akiru isan.
8 Katatu konse ndinapempha Ambuye kuti andichotsere.
8 Mar tounu Regah isan ayoyoban iti yare kakafin biyu’une tabosair isan.
9 Koma anandiwuza kuti, “Chisomo changa ndi chokukwanira, pakuti mphamvu zanga zimaoneka kwathunthu mwa munthu wofowoka.” Choncho ndidzadzitamandira mokondwera chifukwa cha zofowoka zanga, kuti mʼkutero mphamvu ya Khristu ikhale pa ine.
9 Baise ayu isou eo, “Ayu au manaw kabeber o isa i karam, Ayu au fair i iyab teriririm fair ebitih.” Isan imih ayu boro ana’ora’ara’at aniyasisir gagamin na’in ayu ariririm isan, saise Keriso ana fair tafu namara’at.
10 Tsono, chifukwa cha Khristu, ndimakondwera pamene ndili wofowoka, pamene akundinyoza, pamene ndikumva zowawa, ndi pamene akundizunza ndi kundisautsa. Pakuti pamene ndili wofowoka ndiye kuti ndili wamphamvu.
10 Nati isan Keriso wabinamaim ariririm baise abiyasisir, tur kakafin, bowabow fokarih, yawas o morob, yare ta ta fokarih. Anamaramaim ariririm ayu fair abaib.
11 Ndadzisandutsa wopusa, koma inu mwandichititsa zimenezi. Ndinu amene munayenera kundichitira umboni. Ngakhale kuti sindine kanthu, koma sindine wochepetsetsa kwa “atumwi apamwamba” aja.
11 Ayu au sinaf i boun hai not meyemeye na’atube, baise kwa kwa’ora’ahu ayu anasinaf. Kwa karam ayu isou boro baibasit tur kwatao, anayabin ayu i men kafa’imo orot fairu boun iti tounamatar hai fair gagamih na’atube, ayu i yabin en.
12 Ndinapirira pokuonetserani zizindikiro za mtumwi weniweni, pochita pakati panu zizindikiro, zodabwitsa ndi ntchito zamphamvu.
12 Anamaramaim ayu bairit tama’am, ayu yataunub naatu ina’inan, men tisinaf emamatar asinaf himatar naatu baifofofor fairih maiyow kwa wanawanamaim asinaf himatar, iti ebiturobe ayu i kwa a turabarayan.
13 Kodi inu munaoneka ochepa motani ku mipingo ina, kupatula kuti sindinali cholemetsa kwa inu? Mundikhululukire cholakwa chimenechi!
13 Ayu au sinaf mi’itube isa asisinaf i na’atube ekalesia sabuw etei isah a sisinaf. Ana veya ta ayu men kafa’imo ubar aitimih kabay yai’in ayu baibaisu isan. Abistan kakafin asisinaf kwaninatbuhuruwu.
14 Ndakonzeka tsopano kudzakuyenderani kachitatu, ndipo sindidzakhala cholemetsa kwa inu chifukwa ndikungofuna inuyo osati zinthu zanu. Pakuti ana sasamalira makolo koma makolo ndiwo asamalira ana.
14 Iti boun i mar baitounin ayu abobogaigiwas anan kwa aninanawani. Ayu au naa isan boro men aniwa’an nafokar anayabin ayu men akokok kwa a sawar, ayu akokok i kwa. Kek i men karam hinah tamah hinakaifih baise hinah tamah i karam kek hinakaifih
15 Motero ndidzakondwera kukupatsani zanga zonse zimene ndili nazo ndi kudziperekanso ine mwini chifukwa cha inu. Kodi ine ndikamakukondani kwambiri chotere, inuyo mudzandikonda pangʼono?
15 Ayu i abiyasisir gagamin na’in, ayu au sawar etei kwa isa abi’asrouwen naatu au fair etei anit kwa a baibais isan. Kwa isa ayu abi yabow kwanekwan, naatu aisimamih ayu isou men kwabiyabow gewas?
16 Ena mwa inu amavomereza kuti sindinali cholemetsa. Komabe ena amaganiza kuti ndine wochenjera, ndipo ndinakuchenjererani.
16 Isan imih iti tur ao i kwabibasit, ayu men kwa bit ait. Baise sabuw afa boro ayu isou hinao, ayu i ah atain abifufuwen.
17 Kodi ndinakudyerani masuku pamutu kudzera mwa wina aliyense amene ndinamutumiza kwa inu?
17 Ayu oro’orot aiyunih hinanamaim ayu kwa abainuwi?
18 Ndinamupempha Tito kuti abwere kwanuko ndipo ndinamutumiza pamodzi ndi mʼbale wathu. Kodi kapena Tito anakudyerani masuku pamutu? Kodi iye ndi ine sitinachite zinthu mofanana ndi Mzimu mmodzi yemweyo?
18 Ayu Titus aifefeyan i boro tuwat ta hairi hinan kwa hininanawani.
19 Kodi mukuyesa kuti nthawi yonseyi takhala tikudzitchinjiriza tokha? Takhala tikuyankhula pamaso pa Mulungu monga anthu amene ali mwa Khristu; ndipo abwenzi okondedwa, chilichonse chimene timachita ndi chofuna kukulimbikitsani.
19 Kwa a not iti na’atube kwanotanot, aki mar etei asisinaftobon aki kwa anarufafari. Aiyabin! Keriso bibinanube aki abibinan, i aki awaimaim eo re God nanamaim aki tur ao’orerereb. Are au ofonah, sawar etei asisinaf, i kwa nibaisi isan.
20 Pakuti ndikuona kuti pamene ndibwera sindidzakupezani monga mmene ndikufunira kuti muzikhalira, ndipo simungadzandione monga mmene mukufunira kundionera. Ndikuopa kuti pangadzakhale mkangano, nsanje, kupserana mitima, kugawikana, ugogodi, miseche, kudzitukumula ndi chisokonezo.
20 Ayu abirubir ana maramaim anan kwa anabinanawani, kwa a itinin i men ayu anotanot na’atube ana itimih naatu ayu kwana i’itu men kwa kwanotanot na’atube kwana itu. Ayu biyau ekakameyaw anayabin nati’imaim gamin ema’am, bobowen, yaso’ar etit erara’iy, kabat, bai’i’iyab, rarikasar, naatu hai ma men gewasih.
21 Ndikuopa kuti pamene ndidzabwerenso, Mulungu adzandichepetsa pamaso panu, ndipo ndidzamva chisoni ndi ambiri amene anachimwa kale ndipo sanalape zonyansa, zachigololo ndi zilakolako zoyipa zimene anachita.
21 Ayu abirubir anamaramaim anan biya ana titit maiye, kwa namaim ayu au God boro au yawas nayara’iy naham, naatu sabuw moumurih marasika kakafih hisisinaf isan boro anarererey. Anayabin kwa i dogoroh kato men kwainatbuhuruwen, naatu baiwa’an ana bainikinik. I boro’ika kwama kwabi’a’it.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 12, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.