2 Coríntios 10

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Mwa kufatsa ndi kuleza mtima kwa Khristu, ndikukupemphani, ine Paulo amene anthu ena amati ndimachita manyazi tikaonana maso ndi maso ndi inu, koma wosaopa pamene ndili kutali nanu!
1 Kwa sabuw afa ayu isou iti na’atube kwao, anamaramaim Paul bairit tama’am i ebirubir naatu tur hamenamo eo, naatu ef yok enanan mar etei eo’ofokafok, baise Keriso ana yara’iyen naatu ana kakafemaim ayu Paul kwa isa abifefeyan.
2 Ndikukupemphani kuti ndikadzafika kumeneko ndisadzachite kuyankhula mwamphamvu monga mmene ndimayembekezera kudzachita kwa anthu ena amene amaganiza kuti machitidwe athu ndi ofanana ndi anthu a dziko lapansi.
2 Ayu anamaramaim anan biya anatit, kwana’itin gewas sabuw afa it tafaram ana yawasamaim ma hirouw te’o isah boro tur fokarin anao.
3 Ngakhale ife timakhala mʼdziko lapansi, sitimenya nkhondo monga mmene dziko lapansi limachitira.
3 Iti i anababatun it i tafaramamaim tama’am, baise it men tafaram ana yawasamaim tabiyowamih.
4 Pakuti zida zathu zankhondo si zida za dziko lapansi. Koma ndi mphamvu zochokera kwa Mulungu zotha kugwetsa malinga.
4 Aki baiyow ana sawar imaim abiyow i men tafaram ana baiyow sawaramaim abiyowamih, baise God ana baiyow sawar fairin imaim abiyow menamaim rakit ana fur fokarin ear ebatabat arab atafufufur erara’iy abi’afiy. Menamaim gamin baifufuwen aki arun tufuw emamatar.
5 Timagonjetsa maganizo onse onyenga ndiponso kudzikuza kulikonse kolimbana ndi anthu kuti asadziwe Mulungu. Ndipo timagonjetsa ganizo lililonse kuti limvere Khristu.
5 Aki not baifufuwen naatu kaser hai tur imaim sabuw futih God men tisusu’ub gewas i boun arouw agugurusen. Anayabin nati sabuw not kakafih ana dibur hirun tema’am abotaitih arumutufurih Keriso hinabosiyasiyar isan.
6 Ndipo ife tidzakhala okonzeka kulanga aliyense wosamvera ngati inuyo mutakhala omvera kwenikweni.
6 Aki abogaigiwas sawar ama akakaif, o yait fanai inasasair ef ta ta inasisinaf o boro baimakiy inab. Ai tur etei kwanabobosiyasiyar, aki marasika abogaigiwas sawar iyab aki fanei tesasair boro baikwatutunen anitih.
7 Inu mukuweruza potengera zimene maso anu akuona. Ngati wina akutsimikiza kuti ndi wake wa Khristu, iye aganizenso kuti ifenso ndife a Khristu monga iye.
7 Kwa sawar ufun ana itinin akisin kwa’i’itin. O yait ta kunotanot o akisimo i Keriso nowan, naatu i nanot maiye. Aki i Keriso nowan aki abowabow men kwa kwabowabow na’atube.
8 Tsono ngakhale nditadzitama momasuka za ulamuliro umene Ambuye anatipatsa woti tikukuzeni osati kukuwonongani, ndithu sindidzachita manyazi.
8 Anayabin, iti Regah fair biti ayu gagaminaka isan aora’ara’at, biti i kwa wowabi yen isan men tarabouni ra’iy isan, nati isan ayu men biyu’e’o’ohow.
9 Ine sindikufuna kuoneka ngati ndikukuopsezani ndi makalata anga.
9 Ayu fef akirum enan i men kwa baibiruw isan.
10 Pakuti ena amati, “Makalata ake ndi awukali ndi amphamvu koma maonekedwe a thupi lake ndi wosagwira mtima ndipo mayankhulidwe ake ndi achabechabe.”
10 Sabuw afa iti na’atube te’o, “Paul ana fef i fokarih naatu buriburih, baise anamaramaim bairi abidubur, i eriririm naatu men tur ta eo.”
11 Anthu oterewa ayenera kuzindikira kuti zomwe timalemba mʼmakalata tili kutali ndi zomwe tidzakhale tili komweko.
11 Sabuw nati na’atube i hinaso’ob gewas, abistan fefemaim ao akikirum boro anasinaf hina’itin.
12 Sitikudziyika kapena kudzifananiza tokha ndi anthu ena amene amadziyenereza okha. Pamene akudzifanizira okha podziyerekeza ndi anzawo a mʼgulu lawo lomwe, ndi opanda nzeru.
12 Sabuw iyab i taiyuwih isah tenotanot kwanekwan, aki men kafa’imo bairi abita’ayomih. I taiyuwihiwat tefufunih naatu i taiyuwihiwat hai sinafumaim tebibabatiyih nati sabuw i hai not meyemeye.
13 Komabe, ifeyo sitidzitama modutsa malire ake enieni, koma kudzitama kwathu kudzalekeza mʼmalire amene Mulungu anatiyikira, malire ake ndi mpaka kwa inu.
13 Sabuw afa tesisinaf aki men i isah ao’ora’ara’at. Aki baise bowabow abistan Regah biti i anabow, iti bowabow i na kwa auman iwani.
14 Pakuti sitikudzitama modutsa malire ngati kuti sitinafike kwa inu, popeza tinali oyamba kufika kwa inu ndi Uthenga Wabwino wa Khristu.
14 Aki ora’ara’at i men atetetebon, anafofoninamaim ao’ora’ara’at. Men atan biya atatitit na’at, baise aki anafofonin ana kwa biya atit Keriso ana tur gewasin a binan, nati i an gagamin.
15 Choncho sitinyadiranso ntchito imene ena anayigwira. Chiyembekezo chathu nʼchakuti, pamene chikhulupiriro chanu chikukulirakulira, dera lathu la ntchito pakati panu lidzakulanso kwambiri,
15 Sabuw afa hibow tetetebon, aki i isah men ao’ora’ara’at. Aki anafofoninamaim ai bowabow abowabow i akisinamo isan a’o’ora’ara’at.
16 kuti tikalalikire Uthenga Wabwino mu zigawo zina kupitirira kwanuko. Pakuti sitikufuna kudzitama pa ntchito yogwira ena kale mʼdera la munthu wina.
16 Imih aki boro kwa efan menamaim kwama’ama i anafofoninamaim tur gewasin anabinan. Anayabin aki men akokok sabuw marasika tafaram afa imaim hima hibowabow isah a’o’ora’ara’atamih.
17 Koma, “Ngati munthu akufuna kunyadira, anyadire mwa Ambuye.”
17 Baise God ana Buk Atamanin hikirum hio, “Yait ekokok ora’ara’at, Regah abistan sisinaf i akisinamo naora’ara’ah.”
18 Pakuti munthu amene amavomerezedwa, si amene amadziyenereza yekha, koma munthu amene Ambuye amuyenereza.
18 Anayabin Regah akisinamo it isat enotanot naatu it men taiyuwit isat tanao’ra’ara’at, baise God eo bibasit i akisinamo isan tanaora’ara’at.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 2 Coríntios 10, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.