1 Tessalonicenses 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Nʼchifukwa chake pamene sitinathenso kupirira, tinaganiza kuti kunali bwino kuti atisiye tokha ku Atene.
1 Aki na itimih abiwa’an ef etei hifokar, yomaninamaim tunrabi. Imih ai not abogaigiwas Athens imaim boro akisi anama.
2 Tinatuma Timoteyo, mʼbale wathu ndi mnzathu wogwira naye ntchito ya Mulungu yofalitsa Uthenga Wabwino wa Khristu, kuti adzakulimbitseni mitima ndi kukukhazikitsani mʼchikhulupiriro chanu,
2 Baise, tai Timothy God ana akir wairafin orot ta, Keriso ana Tur Gewasin faramayan, kwa isa abiyafar nan a baitumatum isan koufair nit naatu baibais auman nit.
3 ndi cholinga chakuti wina asasunthike ndi mavutowa. Inu mukudziwa bwino lomwe kuti ndife oyenera kukumana ndi zimenezi.
3 Saise bai’akir kakafin nanan ana veya kwa boro men yait ta a uma hina’oror iti baitumatum inihamiy au’uf inabatamih. Kwa taiyuw kwaso’ob, it i bai’akir kakafin wanawanan runamih tanan.
4 Kunena zoona, pamene tinali nanu, tinkakuwuzani kuti tidzayenera kuzunzidwa. Ndipo monga mukudziwa bwino, zimenezi zinachitikadi.
4 Bairi tama’am ana veya matan fufur aimatnuwi atur ao’owen i kwananot, it boro bai’akir kakafin wanawanan tanarun. Naatu boun i nati emamatar kwana’itin kwanaso’ob.
5 Nʼchifukwa chake, pamene sindikanathanso kupirira, ndinatuma Timoteyo kuti adzaone mmene chikhulupiriro chanu chilili. Ndinkaopa kuti mwina wonyengayo, wakunyengani mʼnjira ina yake ndi kuti ntchito zathu zasanduka zosapindula.
5 Anayabin iti isan ayu anot au yababan ra’at, tai Timothy kwa a baitumatum itinin so’ob isan nati ai yafar na. Ayu abir Routobonayan ef ta’ane narurutubuni na’at, aki ai bowabow etei boro nan yabin en namatar.
6 Koma tsopano Timoteyo wabwera kuchokera kwanuko ndipo watibweretsera nkhani yabwino ya chikhulupiriro chanu ndi chikondi chanu. Iye watiwuzanso kuti masiku onse mumatikumbukira mokondwa, ndipo kuti mumafunitsitsa kutionanso, monga momwe ifenso timalakalakira kukuonani inuyo.
6 Baise Timothy kwa biyane i matabir maiye na aki biyai titaka, kwa a baitumatum naatu mi’itube kwama kwabiyabow ana tur gewasin baina eo anowar, mar etei ai yumat itin isan kwanot kwakakaibaban auman eo anowar. Aki ai kok kwa itimih anot ao na’atube kwabo kwanotanot.
7 Motero abale, mʼmasautso ndi mʼmazunzo athu onse, chikhulupiriro chanu chatilimbikitsa.
7 Isan imih taitu tuwai’inah, bai’akir kakafin wanawanan biyababan abai naatu ai not hikwakwaris ana veya kwa abaitumatumamaim aki koufair abai.
8 Ife tsopano tili moyodi, pakuti mukuyima molimbika mwa Ambuye.
8 Kwa a baitumatum Regah wanawananamaim kwabukikin kwabatabat ana tur anonowar i ai yasisir, imih aki bounabo boro anama gewas.
9 Tingathe bwanji kuyamika Mulungu mokwanira poona chimwemwe chonse chimene tili nacho pamaso pa Mulungu wathu chifukwa cha inu?
9 Aki boro mi’itube God ana merar anay kwa isa, aki ai yasisir dogorei wanawanan i ra’at kwanekwan, a tur anonowar ana veya God nanamaim abiyasisir.
10 Usana ndi usiku timapemphera ndi mtima wonse kuti tionanenso nanu, ndi kukwaniritsa zimene zikusowa pa chikhulupiriro chanu.
10 Naatu dogorei tutufin etei fai mar ayoyoyoban mi’itube atinanawani maiye. Naatu a baitumatum menane ere’er ine baibais atit.
11 Tikupempha kuti Mulungu ndi Atate athu mwini, ndi Ambuye athu Yesu, atikonzere njira yabwino kuti tidzafike kwanuko.
11 Boun au yoyobanamaim mi’itube ata God it Tamat taiyuwin naatu ata Regah Jesu ai ef hitayabuna atan kwa biya atatit.
12 Ambuye achulukitse chikondi chanu ndi kuti chisefukire kwa wina ndi mnzake ndiponso kwa wina aliyense, monga momwe chikondi chathu chichitira kwa inu.
12 Au yoyoban ta i mi’itube ata Regah kwa a yabow tafan taya’abar, taiyuw wanawanamaim yabow takarsuwai, naatu sabuw tutufin etei auman dogoroh wanawanan yabow awan takaratan, kwa isa abiyabow na’atube.
13 Iye alimbikitse mitima yanu kuti mukhale opanda cholakwa ndi oyera mtima pamaso pa Mulungu ndi Atate athu pamene Ambuye athu Yesu akubwera ndi oyera ake onse.
13 Ayoyoyoban maiye mi’itube ata Regah dogor wanawanan koufair nit, naatu nayasairi a ubar en God Tamat nanamaim kakafiyi kwanabat, ata Regah Jesu ana sabuw kakafiyih bairi hinanan ana veya.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Tessalonicenses 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.