1 Timóteo 1
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwa lamulo la Mulungu, Mpulumutsi wathu ndiponso Khristu Yesu chiyembekezo chathu.
1 Ayu Paul, Keriso Jesu ana tur abarayan, naatu God ata baiyawasenayan fair itu naatu iyunu atit Keriso wanawananamaim ata baitumatum itutut imaim nuhit fot tama’am i afafaram.
2 Kwa Timoteyo mwana wanga weniweni mʼchikhulupiriro.
2 O Timothy isa iti fef akikirum, ayu natu anababatun baitumatumayan. Isa ayoyoyoban baiwanbabanen, manaw kabeber, tufuw Tamat God naatu ata Regah Keriso Jesu’une isa nama.
3 Monga ndinakupempha pamene ndinkapita ku Makedoniya, khala ku Efeso komweko kuti uletse anthu ena kuphunzitsa ziphunzitso zonyenga,
3 Ayu o aihamiy au Masedonia anan ana veya, o au’uwi na’atube Ephesus imaim inama saise sabuw afa o iso’obaka ina’uwih baifuwen tur sabuw tibi’obaibiyih hinihamiyen,
4 kapena kumangoyika mitima pa nthano zopeka ndi kufufuza za mayina a makolo awo. Zinthu zotere zimapititsa mʼtsogolo mikangano mʼmalo mwa ntchito ya Mulungu yomwe ndi ya chikhulupiriro.
4 binanakwar hai yabih en naatu hai a’agir hai gin teyowayow i hinihamiyen, anayabin nati turamaim gamin emamatar, naatu men yait ta ibais baitumatumamaim God ana bowabow ebowabowamih.
5 Cholinga cha lamuloli ndi chikondi, chomwe chimachokera mu mtima woyera, chikumbumtima chabwino ndi chikhulupiriro choona.
5 Iti roube’aten tur ana’an gagamin i yabow, imih sabuw ini’obaiyih yabow hinaso’ob gewas, dogoroh naniyan hinab kakafin gewasin hairi hinakusib gewas naatu baitumatum anababatun auman hinaso’ob gewas.
6 Anthu ena anapatuka pa zimenezi ndipo anatsata nkhani zopanda tanthauzo.
6 Sabuw afa sinaf iti gewasih i hihamiyen, naatu tur hai yabih en hibow imaim hio tebowabow.
7 Iwo amafuna kukhala aphunzitsi amalamulo, koma sadziwa zimene akunena, kapena zimene akufuna kutsimikiza.
7 Tekokok ofafar ana bai’obaiyenayah hinamatar, baise men hiso’ob abisa isan teo, naatu abisa isan hifair teo ana’an i men hiso’ob gewas.
8 Tikudziwa kuti Malamulo ndi abwino ngati munthu awagwiritsa ntchito bwino.
8 It taso’ob ofafar i gewasin ana efamaim tana sisinaf na’at.
9 Tikudziwanso kuti Malamulo sakhazikitsidwa chifukwa cha anthu olungama, koma ophwanya lamulo ndi owukira, osaopa Mulungu ndi ochimwa, wopanda chiyero ndi osapembedza; amene amapha abambo awo ndi amayi awo, kapena anthu ena.
9 Taso’ob auman ofafar i men sabuw gewasih isah, baise sabuw ofafar asto’obenayah, tafa’asar, bowabow kakafih sinafuyah, God men hisusu’ub, kakafiyinamaim ma’atih, baitafaror atih, hinah tamah asabunuwayah, sabuw asabunuwayah,
10 Malamulo amayikidwa chifukwa cha anthu achigololo ndi ochita zadama ndi amuna anzawo, anthu ogulitsa akapolo, abodza ndi olumbira zabodza, ndi ochita chilichonse chotsutsana ndi chiphunzitso choona.
10 turahinah a’awah ufuh nayah, oro’orot taiyuwih naatu baibin taiyuwih baisesebar kwanekwaneyah, sabuw bain tobonayah, baifufuwenayah naatu kautabitabirayah isah. Naatu sawar afa kakafih hai sinafumaim iti bai’obaiyen gewasin anababatun ebi’ib.
11 Chiphunzitso chimene chimagwirizana ndi Uthenga Wabwino wonena za ulemerero wa Mulungu wodala, umene Iye mwini anandisungitsa.
11 Nati bai’obaiyen i Tur Gewasin God baigegewasinayan naatu marakaw ana God ayu itutumu bitu i wanawananamaim ema’am.
12 Ndikuthokoza Khristu Yesu Ambuye athu, amene anandipatsa mphamvu pa ntchitoyi. Iye ananditenga kukhala wokhulupirira, nandipatsa ntchito mu utumiki wake.
12 Ayu Keriso Jesu ata Regah ana merar ayiy, au bowabowamaim fair itu. Anayabin fufufunu ayu i bosunusunubayan, imih ana bowabow isan rubinu.
13 Ngakhale kuti kale ndinali wachipongwe, wozunza ndi wankhanza, anandichitira chifundo chifukwa ndinkachita mwaumbuli ndi mopanda chikhulupiriro.
13 Basit ayu marasika i bai’ibayan, gamin baiyowayan, naatu yau so’aso’arin, baise ayu kabibiru, anayabin ayu men aso’ob abisa asisinaf, naatu au baitumatum en.
14 Chisomo cha Ambuye athu chinatsanulidwa pa ine mochuluka, pamodzi ndi chikhulupiriro ndi chikondi zimene zili mwa Khristu Yesu.
14 Ata Regah manaw kabeber ayu tafau yan isuwai re awan karatan, naatu baitumatum yabow hairi ata Regah Jesu Keriso wanawananamaim ayu itu.
15 Mawu odalirika ndi woyenera kuwavomereza kwathunthu ndi awa: Yesu Khristu anabwera pa dziko lapansi kudzapulumutsa ochimwa, ndipo mwa iwowo ine ndiye wochimwitsitsa.
15 Iti tur i tur anababatun kwanitumatum, Keriso Jesu i sabuw hai kakafihine baiyawasih isan tafaramamaim na, naatu sabuw wanawanahimaim ayu i kakafu anababatun.
16 Ndipo pa chifukwa chimenechi, Mulungu anandichitira chifundo, kuti mwa ine, wochimwitsitsa, Khristu Yesu aonetse kuleza mtima kwake konse kuti ndikhale chitsanzo cha omwe angathe kumukhulupirira ndi kulandira moyo wosatha.
16 Ana’an nati isan God ayu kabibiru, saise ayu kakafu anababatun wanawana’umaim Keriso Jesu ana yatenub tutufin etei sabuw iyab boro hinabitumatum ti’obaiyih hita’itin hitan ma’ama wanatowan hitab.
17 Tsopano kwa Mfumu yamuyaya, yosafa, yosaoneka, amene Iye yekha ndiye Mulungu, kukhale ulemu ndi ulemerero mpaka muyaya. Ameni.
17 Naatu wanatowan ana aiwob, morob atin, wa’iwa’irin, God ta’imon, i akisinamo tanifai, naatu tanabora’ara’ah wanatowan, wanatowan! Amen.
18 Mwana wanga Timoteyo, ndikukupatsa langizo ili molingana ndi maulosi amene aneneri ananena za iwe. Pamene ukumbukira mawu amenewa udzatha kumenya bwino nkhondo
18 Timothy ayu natu, iti raube’aten tur abit i abisa marasika dinab o isa hio hairi ta’imon, saise iti tur ini’ufunun baiyow gewasin iniyow,
19 utagwiritsitsa chikhulupiriro ndi chikumbumtima chabwino. Ena anazikana zimenezi motero chikhulupiriro chawo chinawonongeka.
19 baitumatumamaim inabat anot narerekab gewas. Anayabin sabuw afa hai not men rererekab hai baitumatum hibai hin ar koun hiyen hikufufufur.
20 Ena mwa amenewa ndi Humenayo ndi Alekisandro, amene ndinawapereka kwa Satana kuti aphunzire kusachita chipongwe Mulungu.
20 Wanawanahimaim i orot rou’ab Haimeneus naatu Alexander hairi, ayu Satan umanamaim aya saise hinaso’ob God isan men hinigigim.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Timóteo 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.