1 Pedro 4
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Popeza kuti Khristu anamva zowawa mʼthupi lake, mukhale nawonso mtima omwewo, chifukwa iye amene wamva zowawa mʼthupi lake walekana nawo uchimo.
1 Isan imih Keriso i biyanamaim biyababan bai morob, imih not nati ta’imonamaim kwanabogaigiwas biya nababan, anayabin orot biyan baban ebi’akir bowabow kakafin i biyanamaim boro na’afuw.
2 Chifukwa cha ichi, iwo sakhalanso moyo wawo akuchita zofuna za matupi awo, koma amachita chifuniro cha Mulungu.
2 Naatu ana ma nati’imaim nabubusuruf boro men biyan ana kokomaim nabonawiy nama’amih, baise boro God ana kokomaim nama.
3 Pakuti mwataya kale nthawi yambiri mʼmbuyomu pochita zimene anthu osapembedza amachita, moyo wokhumba zonyansa, zilakolako zoyipa kuledzera, zochitika zoyipa za pa phwando, mapokoso ndi kupembedza mafano onyansa.
3 Anayabin kwa veya manin maiyow Eteni Sabuw hai ma na’atube kwama, ayawas etei i kwabisesebar kwanekwan, baiwa’an isan kukura’ara’hi, kwatomatom kwanekwan, ben kawasa wanawanan kwatom kwararowabon, hiyuw kakafih wanawanan kwasisinaf kwanekwan, naatu hai kwafiren kakafih wanawanan kwaikofanih bairi kwakwafir.
4 Anthu osapembedza amadabwa pamene simuthamangira nawo kuchita zoyipitsitsazi, nʼchifukwa chake amakuchitani chipongwe.
4 Turobe kwa a’ofonah bairi marasika kwabita’ay i tibifofofor men kafaita, anayabin abisa kakafin tisisinaf kwabikofanih isan tur kakafih maiyow ti’u’uwi.
5 Koma adzafotokoza okha mlandu wawo kwa Mulungu amene wakonzeka kuweruza amoyo ndi akufa.
5 Baise kwanaso’ob, God sabuw etei boro nibabatiyih, sabuw yawayawasih naatu murumurubih etei. Imih i boro God nanamaim hinabat nabibatiyih hiniya futifut.
6 Pa chifukwa chimenechi, Uthenga Wabwino unalalikidwa ngakhale kwa iwo amene tsopano ndi akufa, kuti adzaweruzidwe monga anthu ku thupi, koma adzakhale ndi moyo monga mwa Mulungu mu mzimu.
6 Ana’an iti isan tur gewasin hibinan, naatu murumurubih auman isah hibinan. Saise biyahine bai’akir hibai himomorob, ayubihine boro yawasih God bairi hinama.
7 Chimaliziro cha zinthu zonse chili pafupi. Choncho khalani maso ndi odziletsa kuti muthe kupemphera.
7 Tafaram ana yomanin i na iyubin. Isan imih anot etei naruboun kwanayamutufuri gewas kwanayoyoban.
8 Koposa zonse muzikondana wina ndi mnzake kwambiri, chifukwa chikondi chimaphimba machimo ambiri.
8 Sawar etei tafahimaim, a yabow dogor babanika taituwa bairi kwaniyabowbonen, anayabin yabow i bowabow kakafih etei esusuma’ay.
9 Muzisamalirana wina ndi mnzake osamanyinyirika.
9 A bar etawan kwanabotawiy a ofonah isah, eremerarayow men eregamin.
10 Aliyense agwiritse ntchito mokhulupirika mphatso iliyonse imene anayilandira potumikira ena ngati adindo ogwiritsa bwino ntchito mphatso za Mulungu za mitundumitundu.
10 Kwa ta’ita’imon God biyanane a siwar ta ta kwabaib, i kwanakaif gewas, taituwa kwanibaisih, saise God ana gewasin kwa wanawanane natit sabuw hina’itin.
11 Ngati wina ayankhula, ayankhuledi mawu enieni a Mulungu. Ngati wina atumikira, atumikire ndi mphamvu imene Mulungu amapereka, kuti pa zonse Mulungu alemekezedwe mwa Yesu Khristu. Kwa Iye kukhale ulemerero ndi mphamvu mpaka muyaya, Ameni.
11 O yait tur o isan ana siwar ibaib, tur inao ana’itinin i God o wanawananamaim eo, o yait baibais ana siwar ibaib, God ana fair bitimaim inabow, saise o a bowabow nati’imaim God boro merarayow hinitin Jesu Keriso wabinamaim. Fair, marakaw i akisinamo isan nama wanatowan, wanatowan. Amen.
12 Abale okondedwa musadabwe ndi mayesero owawa amene mukukumana nawo ngati kuti china chake chachilendo chakuchitikirani.
12 Are au ofonah, men kwana’oror iti routobon kakafin wanawanan kwarun e’a’arahih isan, ana’itin boun sawar asir isa emamatar na’atube.
13 Koma kondwerani popeza mukumva zowawa pamodzi ndi Khristu, kuti mudzakondwere kwakukulu pamene ulemerero wake udzaonekera.
13 En baise, kwaniyasisir, kwa i Keriso ana bai’akir turin kwabaib, saise i ana fair bonamanamarin nabirerereb anamaramaim kwa boro dogor yasisir awan nakaratan.
14 Ngati akuchitani chipongwe chifukwa cha dzina la Khristu, ndinu odala, ndiye kuti Mzimu waulemerero wa Mulungu uli pa inu.
14 Keriso wabinamaim sabuw tur kakafih hinao hinabi’a’afiyi boro baigegewasin kwanab, anayabin Ayubin gewagewasin, God Anun Kakafiyin i kwa tafa mara’at ema’am.
15 Ngati mumva zowawa, zisakhale chifukwa cha kupha munthu, kapena kuba, kapena kuchita choyipa, kapena kulowerera za anthu ena,
15 Kwai’akir biya ebababan i men sabuw kwa’a’asbunubunuw, o kwababain isan, kakafih kwasisinaf isan, o sabuw hai wau kwayiy isan.
16 koma ngati mumva zowawa chifukwa ndinu Mkhristu, musachite manyazi, koma muyamike Mulungu chifukwa cha dzinalo.
16 En baise kwai’akir biya ebababan, anayabin kwa i Kirisiyan sabuw, imih men biya na’ohow, baise God kwanabora’ara’ah ana merar kwanay, bai’akir nati na’atube wabinamaim kwabaib isan.
17 Pakuti nthawi yafika kuti chiweruzo chiyambe mʼnyumba ya Mulungu, ndipo ngati chiyamba ndi ife nanga podzafika kwa osamvera Uthenga Wabwino wa Mulungu, chidzakhala chotani?
17 Baibatebat ana veya i etitit, naatu God natunatun i boro wan nibabatiyih. Naatu it Kirisiyan sabuw auman boro nibabatiyit, baise sabuw iyab God ana Tur Gewasin men hibitumatum yomaninamaim isah boro abisa namatar?
18 Monga Malemba akuti,
18 Buk Atamaninamaim eo,
19 Nʼchifukwa chake, iwo amene akumva zowawa monga mwa chifuniro cha Mulungu, adzipereke okha mʼmanja mwa Mlengi wawo wokhulupirika ndi kumapitiriza kuchita zabwino.
19 Isan imih sabuw iyab God ana kokomaim tibi’akir, hai sinaf gewasinamaim God hai Baimatarenayan hinitumitum, anayabin God ana omatanen i mar etei esinaf tibiturobe.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Pedro 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.