1 Pedro 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Choncho, lekani zoyipa zonse, chinyengo chilichonse, chiphamaso, nsanje ndi kusinjirira kulikonse.
1 Isan imih yawas kakafih boro kwanihamiyen. Men kwanifuwen, men awa hinaharewan, men kwanibobowen, men turanah isah tur kakafin kwanao.
2 Monga makanda obadwa kumene amalirira mkaka, inunso muzilakalaka mkaka weniweni wauzimu, kuti mukule ndi kukufikitsani ku chipulumutso chanu,
2 Kek sosof na’atube kwanamatar, mar etei sika namamah ayub ananun tom isan, saise i kwanatomatom kwa ayawas boro nara’at nayen.
3 pakuti tsopano mwalawadi kuti Ambuye ndi wabwino.
3 Buk Atamaninamaim hi’o hikirum, “Kwa taiyuw ayawasamaim kwaso’ob Regah i kabeberayan.”
4 Pamene mukubwera kwa Iye, amene ndi Mwala wa moyo, umene anthu anawukana, koma Mulungu anawusankha kuti ndi wa mtengowapatali,
4 Kwana ata Regah biyanaika kwanama, iti kabay yawasin sabuw hi’itin hikwahir yabin en hirouw, baise God rubin na mokob foun matar.
5 inunso, mukhale ngati miyala ya moyo yoti Mulungu amangire nyumba yake yauzimu kuti mukhale ansembe opatulika, opereka nsembe zauzimu zovomerezeka ndi Mulungu mwa Yesu Khristu.
5 Kwa baitumatumayah i wabat wanatowanin na’atube, imaim God bai ayub ana Tafaror Bar ewowowab. Kwa auman i firis ana kou’ay ayubitane ana sibor kwaya’ay. Jesu Keriso ana baibaisamaim, God i iyasisir ebaib.
6 Pakuti mʼMalemba mwalembedwa kuti,
6 Buk Atamaninamaim iti na’atube hikirum,
7 Tsono kwa inu okhulupirira, mwalawo ndi wamtengowapatali. Koma kwa amene sakhulupirira,
7 Kwa iyab kwabitumitum, Keriso i kabay gewasin kwa isa, baise kwa iyab men kwabitumitum isa boro men gewasin.
8 ndi
8 Naatu ibanak Buk Atamaninamaim hikirum hio,
9 Koma inu ndinu anthu osankhidwa ndi Mulungu, ansembe achifumu, mtundu woyera mtima, anthu ake enieni a Mulungu, munasankhidwa kuti mulalikire za ntchito zamphamvu za Iye amene anakuyitanani kuti mutuluke mu mdima ndi kulowa mʼkuwunika kwake kodabwitsa.
9 Baise kwa i God ana rubinen sabuw, kwa i firis gewas, God ana sabuw kakafiyi, naatu God nowan, imih God ana bowabow gewasin kwanaorereb, anayabin guguminamaim kwama’am botaiti kwatit marakaw bonamanamarin gewasin kwabai.
10 Kale simunali anthu ake, koma tsopano ndinu anthu a Mulungu. Kale simunalandire chifundo, koma tsopano mwalandira chifundo.
10 Marasika kwa men God ana sabuw, baise boun kwa i ana sabuw. Marasika God ana kabeber men kwabai, baise boun i ana kabeber kwabai.
11 Okondedwa, ndikukupemphani, ngati alendo pansi pano, pewani zilakolako za uchimo, zimene zimachita nkhondo ndi moyo wanu.
11 Are au ofonah, kwa au’uwi kwa i nanawan naatu touman sabuw na’atube iti tafaramaim kwama’am! Men biya ana kok nabonawiyi imaim nakaifi. Nati biya ana kok i boun rakit na’atube, boro ayub hairi hiniyow.
12 Khalani moyo wabwino pakati pa anthu osapembedza kuti ngakhale atakusinjirirani kuti mumachita zoyipa, iwowo akaona ntchito zanu zabwino, adzalemekeza Mulungu pa tsiku lomwe Iye adzatiyendere.
12 Eteni Sabuw matahimaim kwanakaifi gewas kwanama. Kwa isa boro bowabow kakafih sinafuyah hinarauw hinao, baise anamaramaim bowabow gewasin kwanasisinaf boro men isa tur ta hinao. Imih Baibatebat ana Veya God namamatabir. Kwa isa boro God ana merar hina hinabora’ara’ah.
13 Gonjerani maulamuliro onse chifukwa cha Ambuye. Kaya ndi mfumu, imvereni chifukwa ili ndi ulamuliro waukulu,
13 Regah wabinamaim kwa kwayar’iy sabuw gagamih babahimaim kwanama. Gawan hai aiwob gagamin aiwob etei ukwarih,
14 kaya ndi mabwanamkubwa, pakuti watumidwa ndi mfumu kuti alange onse amene amachita zoyipa ndi kuyamikira onse amene amachita zabwino.
14 gawan sabuw iyab gawan ana ukwarin iyafarih hitit tafaram ta ta tekakaif, imih iyab bowabow kakafin tesisinaf boro hinabow baimakiy hinitih, baise iyab bowabow gewasin tesisinaf boro hinabora’ara’ahih.
15 Pakuti Mulungu akufuna kuti pochita ntchito zabwino muthetse kuyankhula mosazindikira ndi mopusa.
15 God ekokok kwa kwanasinaf gewas saife nati sabuw hai not meyemeye, boro hinanutanubamo hinama, aurih ef men ema’am boro isa tur kakafih hinao.
16 Mukhale monga mfulu, koma musagwiritse ntchito ufulu wanuwo ngati chophimbira zoyipa; mukhale monga atumiki a Mulungu.
16 Kwa ama i sabuw roufamen na’atube kwanama, baise men nati roufamen ana yawasamaim kwama’am isan afair kwanab kakafin kwanasinaf, baise kwa i God ana’akir wairafihibe kwanama.
17 Chitirani ulemu aliyense, kondani abale okhulupirira, wopani Mulungu, ndipo chitirani mfumu ulemu.
17 Sabuw etei isah kwanakakaf. A ofonah baitumatumayah isah kwaniyabow kwanakakaf. Naatu aiwob hai ukwarin isan kwanakakaf.
18 Inu akapolo, gonjerani ambuye anu ndi kuwachitira ulemu, osati kwa iwo okha amene ndi abwino ndi omvetsa zinthu, komanso kwa amene ndi ankhanza.
18 Kwa akir wairafi kakafemaim kwanayara’iy, a orot ukwarih fanah kwanab babahimaim kwanama, men gewasin isa isisinaf akisin fanah kwanab, baise iyab fokarin isa tisisinaf auman fanah kwanab.
19 Pakuti ndi chinthu chokoma ngati munthu apirira mu zowawa zimene sizinamuyenera chifukwa chodziwa kuti Mulungu alipo.
19 Kwa anot tutufin etei God ana kokomaim kwabowabow naatu sabuw asir biyababan hinit nawawainabi isan, God boro nigegewasini.
20 Kodi pali choti akuyamikireni ngati mupirira pomenyedwa chifukwa choti mwalakwa? Koma ngati mumva zowawa chifukwa chochita zabwino ndi kupirira, mwachita choyamikika pamaso pa Mulungu.
20 Bo kakafin kwasisinaf isan hinarab nawawainabi ana gewasin boro abisa kwanab, baise gewasin kwanasinaf isan nawainabi kwabi’akir God boro nigegewasini.
21 Munayitanidwa kudzachita zimenezi, chifukwa Khristu anamva zowawa chifukwa cha inu, anakusiyirani chitsanzo, kuti inu mutsatire mʼmapazi ake.
21 Kwa afa’af kwabai i bai’akir isan, anayabin Keriso kwa isa i’akir ana bai’obaiyen yare saise i an efanin kwani’ufunun.
22 “Iye sanachite tchimo
22 “Bowabow kakafin men ta sinaf,
23 Pamene anthu ankamuchita chipongwe, Iye sanabwezere chipongwe, pamene Iye ankamva zowawa, sanaopseze. Mʼmalo mwake, anadzipereka kwa Mulungu amene amaweruza molungama.
23 Hibi’i’iyab ana maramaim i men kafa’imo bai’iyab tur ta wan yi isah eomih, i bi’akir ana veya men hibiruwimih, baise ana nuhifot i God mutufor baibatiyenayan imaim yai.
24 Iye mwini anasenza machimo athu mʼthupi lake pa mtanda, kuti ife tife kutchimo ndi kukhala ndi moyo potsata chilungamo, ndipo ndi mabala ake munachiritsidwa.
24 Keriso akisinamo ata kakafih i biyanamaim eabar onaf afe’enamaim yen, saise it bowabow kakafinane tanamorob naatu yawas mutuforomaim tanama, i ana fitamaim it iyawasit.
25 Pakuti munali monga nkhosa zosochera, koma tsopano mwabwerera kwa mʼbusa ndi woyangʼanira miyoyo yanu.
25 Anayabin kwa bobaituw sheep na’atube ef kwasa’ir nanabin kwan, baise boun kwa buwi kwamatabir kwana Nabatanenayan naatu anun ana kaifenayan biyan kwatit.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Pedro 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.