1 João 4
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Anzanga okondedwa, musakhulupirire mzimu uliwonse, koma yesani mizimu ngati ikuchokera kwa Mulungu, chifukwa aneneri onama ambiri afalikira mʼdziko lapansi.
1 Are au ofonah, sabuw etei Anun Kakafiyin bain hinarouw hinao men kwanitutumih, baise wantoro’ot kwanafufunih kwana’itin, turobe i God biyanane Anun Kakafiyin hibai ai en. Anayabin dinab baifufuwenayah moumurih maiyow hitit tafaram awan karatan.
2 Mungathe kuzindikira Mzimu wa Mulungu motere: Mzimu uliwonse umene umavomereza kuti Yesu Khristu anabwera mʼthupi, ndi wochokera kwa Mulungu,
2 Ef i boro iti na’atube kwana’itin kwanaso’ob, nati sabuw i Anun Kakafiyin hibai ai en. Sabuw iyab hina’orereb Jesu i turobe Keriso, naatu orot babin biyah bai. Nati sabuw i turobe Anun Kakafiyin hibai.
3 koma mzimu uliwonse umene suvomereza Yesu, siwochokera kwa Mulungu. Uwu ndi mzimu wa wokana Khristu umene munawumva kuti ukubwera ndipo ngakhale tsopano wabwera kale mʼdziko lapansi.
3 Baise sabuw iyab hina’orereb Jesu i men Godane na, nati sabuw i men Anun Kakafiyin hibaimih. Baise Keriso ana kamabiy orot anunin hibai. Marasika hio kwanowar Keriso ana kamabiy wairafin i boro nan, naatu boun i na tafaram wanawananamaim titaka.
4 Inu ana okondedwa, ndinu ochokera kwa Mulungu ndipo mwawagonjetsa aneneri onyengawa, chifukwa Iye amene ali mwa inu ndi wamkulu kuposa amene ali mʼdziko lapansi.
4 Baise natunatu, kwa i Tamat God nowan, dinab kakafih Keriso isan hibirakit kwawastanih. Anayabin Anun Kakafiyin wanawanamaim ema’am ana fair i ra’at. Tur anababatun ebi’obaiyi, men sabuw iyab iti tafaram ana wagabur hibow tema’am hai fair na’atube’emih.
5 Aneneri onyengawa ndi ochokera mʼdziko lapansi, nʼchifukwa chake amayankhula za dziko lapansi, ndipo dziko lapansi limawamvera.
5 Dinab baifufuwenayah tafaramamaim abisa temamatar isah tibidudur, sabuw iyab iti tafaram nowan tenonowar. Anayabin nati sabuw i tafaram nowan.
6 Ife ndi ochokera kwa Mulungu, ndipo aliyense amene amadziwa Mulungu amamvera zimene timayankhula. Koma aliyense amene sachokera kwa Mulungu samvera zimene timayankhula. Mmenemu ndiye mmene timasiyanitsira pakati pa mzimu wachoonadi ndi Mzimu wachinyengo.
6 Baise iti i God nowan, imih sabuw iyab God hisoso’ob, abisa tao boro hinanowar. Sabuw iyab men God nowan, abisa tao boro men hinanowar. Hai itinin boro iti’imaim tana’itan tana’inanih, menatan i turobe Anun Kakafiyinane enan, naatu menatan i wagabur baifufuwenayanane enan.
7 Anzanga okondedwa, tiyeni tikondane wina ndi mnzake, pakuti chikondi chimachokera kwa Mulungu. Aliyense amene ali ndi chikondi ndi mwana wa Mulungu ndipo amadziwa Mulungu.
7 Are au ofonah, akokok taniyabowbonen, anayabin yabow i Godane enan. Orot babin yait ebiyabow, i God nowan naatu God su’ub.
8 Aliyense amene alibe chikondi sadziwa Mulungu, chifukwa Mulungu ndiye chikondi.
8 Anayabin God i yabow wairafin, imih orot babin yait men ebiyabow, i God men su’ub.
9 Mmene Mulungu anaonetsera chikondi chake pakati pathu ndi umu: Iye anatumiza Mwana wake mmodzi yekha ku dziko lapansi kuti mwa Iyeyo tikhale ndi moyo.
9 God ana yabow it i’obaiyit, Natun ta’imonamo tafaramamaim iyun re it isat. Saise i biyanamaim it yawas tatab.
10 Chikondi ndi ichi: osati kuti ife ndife amene tinamukonda Mulungu, koma kuti Iyeyo ndiye amene anatikonda ndipo anatumiza Mwana wake kuti akhale nsembe yopepesera machimo athu.
10 Yabow ana’itininaban i nati, it men God taiyabuw. Baise God it iyabuwit Natun ta’imonamo iyun re, saise ine it ata bowabow kakafih God notawiyen.
11 Anzanga okondedwa, popeza Mulungu anatikonda chotere, ifenso tiyenera kukondana wina ndi mnzake.
11 Are au ofonah, God ana yabow iti na’atube iyabuwit, imih it auman taituwat bairi tatiyabowbonen.
12 Palibe amene anaonapo Mulungu, koma tikakondana wina ndi mnzake, ndiye kuti Mulungu amakhala mwa ife ndipo chikondi chake chafika pachimake penipeni mwa ife.
12 Orot men yait ta God itinimih, baise taituwat bairi tanabiyabowbonen na’at, God boro wanawanatamaim bairit tanama. Naatu i ana yabow boro wanawanatamaim nara’at.
13 Ife tikudziwa kuti timakhala mwa Iye ndipo Iyeyo amakhala mwa ife chifukwa anatipatsa Mzimu wake.
13 Taso’ob it i God wanawanatamaim ema’am, anayabin Anun Kakafiyin it itit.
14 Ndipo taona ndipo tikuchitira umboni, kuti Atate anatuma Mwana wake kuti akhale Mpulumutsi wa dziko lapansi.
14 Naatu iti Anun Kakafiyin naniyan i tatam sabuw afa hai tur ta’o’owen, Tamat i Natun iyun re tafaram ana baiyawasenayan matar.
15 Ngati aliyense avomereza kuti Yesu ndi Mwana wa Mulungu, Mulungu amakhala mwa iye ndipo iyeyo amakhala mwa Mulungu.
15 Orot yait eo’orereb Jesu i God Natun, nati orot boro God hairi hinita’imon.
16 Tikudziwa ndipo timadalira chikondi chimene Mulungu ali nacho pa ife.
16 Isan imih it taso’ob God ana yabow isat ebobotan i tabitumitum. God i yabow wairafin, orot yait yabowamaim ema’am, nati orot wanawananamaim God ema’am, naatu God wanawananamaim i orot ema’am.
17 Chikondi chafika pachimake penipeni pakati pathu, kotero kuti pa tsiku lachiweruzo tidzakhala olimba mtima chifukwa mʼdziko lapansi moyo wathu uli ngati wa Khristu.
17 Yabow ana ef nati na’atube wanawanatamaim nama’am, boro nakusouwit tanan Keriso’obe tanamatar, naatu baibatebat ana Veya boro men tanabir.
18 Mulibe mantha mʼchikondi. Koma chikondi ndi changwiro chimachotsa mantha, chifukwa mantha amabwera chifukwa choopa chilango. Munthu amene ali ndi mantha, chikondi chake sichangwiro.
18 Anababatun yabow wanawanan i men bir ema’am, baise uhewbitan boro bir kakafin nanun nabihir. Anayabin bir i baimakiy isan boro nibibiruwit. Baise yait dogor wanawanan yabow men ema’am o yabow ana ef men iso’ob.
19 Ife timakonda Mulungu chifukwa ndiye anayamba kutikonda.
19 God tabiyabuw, anayabin God mat it iyabuwit.
20 Ngati wina anena kuti, “Ine ndimakonda Mulungu,” koma namadana ndi mʼbale wake ndi wabodza ameneyo. Pakuti aliyense amene sakonda mʼbale wake, amene akumuona, sangathenso kukonda Mulungu amene sanamuone.
20 Orot yait nao, “Ayu God abiyabuw,” baise tain tuwan ebifa’ifai, nati orot i baifufuwenayan. Anayabin nati orot taintuwan itih bairi tema’am, baise men i biyabuwih, naatu God men i’itin boro mi’itube niyabuw.
21 Ndipo Iye anatipatsa lamulo lakuti: Aliyense amene amakonda Mulungu ayenera kukondanso mʼbale wake.
21 Keriso obaiyunen tur eo tanonowar i iti, “Orot babin yait God ebiyabuw, gewasin tain tuwan auman niyabuwih.”
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 João 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.