1 João 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Taonani kukula kwake kwa chikondi chimene Atate anatikonda nacho, kuti titchedwe ana a Mulungu! Ndipo nʼchimene ife tili! Nʼchifukwa chake dziko lapansi silitidziwa chifukwa silinamudziwe Iye.
1 God ana yabow it isat rara’at kwana’itin, ana yabow it isat ra’at, imih God it natunatun rouw ea’afit. It i anababatun God natunatunamih tamatar. Imih iti tafaram ana sabuw men hisu’ubit, na’atube God auman men hisu’ub.
2 Abale okondedwa, tsopano ndife ana a Mulungu, ndipo sichinaoneke chimene tidzakhala. Koma tikudziwa kuti Yesu akadzaonekera, tidzafanana naye, pakuti tidzamuona Iyeyo monga momwe alili.
2 Are au ofonah, it i boun God natunatun tamatar. Baise men isat ibebeyan taso’ob gewas abisa boro isat namatar. Baise Keriso nanan ana veya’amaim it taso’ob, it boro i ana itininabe. Anayabin boro matatyan ana itinin mi’itube boro i na’atube tana’itin.
3 Aliyense amene ali ndi chiyembekezo ichi mwa Iye adziyeretse yekha, monga Iye ali woyera.
3 Isan imih sabuw iyab tibitumatum Keriso boro namatabir maiye, taiyuwih hinaya’asairih dogoroh sasouwin hinama Keriso na’atube.
4 Aliyense amene amachimwa amaphwanya lamulo; pakuti tchimo ndi kuphwanya lamulo.
4 Orot yait bowabow kakafin esisinaf, i God ana ofafar ea’astu’ub, imih ana ubar boro nab. Anayabin bowabow kakafinamaim ofafar ea’astu’ub.
5 Koma inu mukudziwa kuti Yesu anabwera kuti adzachotse machimo athu. Ndipo mwa Iye mulibe tchimo.
5 Keriso ra’iy ata bowabow kakafih bobosairen i kwaso’ob, i aurin i kakafin en.
6 Aliyense wokhala mwa Khristu sachimwa. Aliyense amene amachimwa sanamuone kapena kumudziwa.
6 Imih sabuw iyab Keriso bairi tema’am boro men matan fufur bowabow kakafin hinasinafumih. Baise sabuw iyab matan fufur bowabow kakafin tisisinaf, anayabin Keriso men hi’itin o men hisu’ub.
7 Ana okondedwa, musalole kuti aliyense akusocheretseni. Munthu amene amachita chilungamo ndi wolungama, monga Khristu ali wolungama.
7 Natunatu sabuw men hinikubibiruwi, orot yait ef gewasin esisinaf i ana ef gewasin, Keriso ana ef gewasin na’atube.
8 Iye amene amachimwa ndi wa Satana, chifukwa mdierekezi wakhala akuchimwa kuyambira pa chiyambi. Mwana wa Mulungu anaonekera kuti awononge ntchito za mdierekezi.
8 Orot yait matanfufur bowabow kakafin esisinaf i Demon natun. Anayabin Demon Mowan aneika bowabow kakafin sinaf. Imih God Natun re’er anayabin i abisa Demon biwa’an i gurusinamih raiy.
9 Aliyense amene ndi mwana wa Mulungu, sachimwirachimwira, popeza mbewu ya Mulungu ili mwa iye, sangathe kuchimwa, chifukwa ndi mwana wa Mulungu.
9 Orot yait God Natun, i boro men matanfufur bowabow kakafin nasinafumih. Anayabin God naniyan anababatun i nati orot yan wanawanan ema’am. Imih boro men mar etei bowabow kakafin nasinaf, yabin i Tamah God.
10 Mmenemu ndi mmene timadziwira ana a Mulungu ndi amene ali ana a mdierekezi. Aliyense amene sachita chilungamo si mwana wa Mulungu; ngakhalenso amene sakonda mʼbale wake.
10 Imih God natunatun naatu Demon natunatun hai itinin i bebeyan ta’i’itin. Orot yait men ef gewasin esisinaf, o tain men ebiyabuw nati orot i men God natunamih.
11 Uthenga umene munawumva kuyambira pachiyambi ndi uwu: Tizikondana wina ndi mnzake.
11 Tur aneika hiorereb kwanonowar i baiyabowbonen isan hio.
12 Musakhale ngati Kaini, amene anali wa woyipayo ndipo anapha mʼbale wake. Nanga anamupha chifukwa chiyani? Chifukwa zochita zake zinali zoyipa ndipo zochita za mʼbale wake zinali zolungama.
12 It men Cain na’atube tanasinafumih, anayabin i demon nowan. Aisim tain easabun? Anayabin abisa sisinaf i kakafin, baise tain ana ef i mutufurin, imih men Cain sisinafube kwanasinafumih.
13 Abale anga, musadabwe ngati dziko lapansi lidana nanu.
13 Taitu, iti tafaram ana sabuw hinabifa’ifai men kwanakasiyomih.
14 Ife tikudziwa kuti tinatuluka mu imfa ndi kulowa mʼmoyo, chifukwa timakonda abale athu. Aliyense amene sakonda mʼbale wake akanali mu imfa.
14 Aki aso’ob morob aisnowah arabon yawas ana efamaim abatabat, anayabin taiti abiyabuwih. Orot yait men ebiyabow i morob ana efanika ema’am.
15 Aliyense amene amadana ndi mʼbale wake ndi wakupha, ndipo inu mukudziwa kuti wopha anthu mwa iye mulibe moyo wosatha.
15 Orot yait tain ebifa’ifai i farumayan na’atube imih nati farumayan aurin yawas wanatowan wanawananamaim men ema’am.
16 Mmene timadziwira chikondi chenicheni ndi umu: Yesu anapereka moyo wake chifukwa cha ife. Ndipo nafenso tiyenera kupereka miyoyo yathu chifukwa cha abale athu.
16 Yabow ana ef aki iti’imaim aso’ob. Keriso ana yawas it isat i’inuw, imih it auman taituwat isah ata yawas tani’inuw.
17 Ngati wina ali ndi chuma ndipo nʼkuona mʼbale wake akusowa, koma wosamvera chisoni, kodi mwa iyeyo muli chikondi cha Mulungu?
17 Orot sawar wairafin tain itin ebi’akir baise baibaisin isan men ekokok, nati orot aurin God ana yabow men ema’am.
18 Ana okondedwa, chikondi chathu chisakhale cha pakamwa pokha koma cha ntchito zathu ndi mʼchoonadi.
18 Natunatu yabow i men turawat namomon. Baise yabow i turobe ana itinin auman, saise yabow turobe namatar.
19 Pamenepo tidzadziwa kuti tili pa choonadi ndipo tidzakhala okhazikika mtima pamaso pa Mulungu,
19 Ef iti’imaim it boro tanaso’ob it i anababatun turobe nowan. Naatu God nanamaim boro koufair tanab tanabat.
20 nthawi zonse pamene mtima wathu utitsutsa. Pakuti Mulungu ndi wamkulu kuposa mitima yathu ndipo Iye amadziwa zonse.
20 It dogorot wanawanan abisa kakafin esisinaf boro tanaso’ob, baise God i ra’at dogorot ata naniyan nasair. Imih abisa kakafin tasisinaf etei i so’ob.
21 Anzanga okondedwa, ngati mitima yathu sikutitsutsa, tili nako kulimbika mtima pamaso pa Mulungu.
21 Isan imih au ofonah, dogorot ana naniyan men nabi’afiyit, God nanamaim boro koufair tanab. Naatu abisa takokok isan yoyobanamaim tanifefeyan boro nitit.
22 Ndipo timalandira chilichonse chimene tichipempha kwa Iye, chifukwa timamvera malamulo ake ndi kuchita zimene zimamukondweretsa.
22 Abisa isan tanifefeyan boro tanab, anayabin ana ofafar tabobosiyasiyar, naatu abisa tasisinaf i yan esisisir.
23 Ndipo lamulo lake ndi ili: kukhulupirira dzina la Mwana wake, Yesu Khristu, ndi kukondana wina ndi mnzake monga Iye anatilamulira.
23 Naatu iti i ana obaiyunen tur, Natun Jesu Keriso wabinamaim tanitumatum naatu taniyabowbonen, iyunit eo na’atube.
24 Iwo amene amamvera malamulo ake amakhala mwa Iye, ndipo Iye amakhala mwa iwo. Ndipo mmenemu ndi momwe timadziwira kuti Iye akukhala mwa ife. Timadziwa mwa Mzimu Woyera amene anatipatsa.
24 Sabuw iyab God ana ofafar tebobosiyasiyar, God i wanawanahimaim ema’am, na’atube i wanawananamaim tema’am. Anayabin aki God Anun Kakafiyin biti’imaim a so’ob, God aki wanawananamaim ema’am.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 João 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.