1 Coríntios 5

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Mbiri yamveka kuti pakati panu pakuchitika chigololo. Ndipo chigololo cha mtunduwu ngakhale pakati pa akunja sichingapezeke; munthu akumagonana ndi mkazi wa abambo ake.
1 Tur anonowar kwa wanawanamaim intabitabir baiwa’an kwanekwan i ra’at, Eteni Sabuw iyab God men hisusu’ub bowabow iti na’atube i men tisisinaf. Iti ao anayabin, ayu tur anowar orot ta kwa wanawanamaim i tamah aawan ufuyey hairi ti’inu’in.
2 Ndipo inu mukudzitukumulabe. Kodi simukanayenera kudzazidwa ndi chisoni ndipo mukanamuchotsa pa chiyanjano chanu munthu wochita zimenezi?
2 Naatu kwa aisim kwabi’o’orot? Ana gewasin kwatiyababan kwatarerey, orot nati bowabow kakafin sisinaf a kou’ayomaim kwatabotait.
3 Ngakhale sindili nanu mʼthupi, ndili nanu mu mzimu. Ndipo ineyo ndapereka kale chiweruzo pa munthu amene amachita zotere, ngati kuti ndili komweko.
3 Ayu biyau’umaim i ef yok ama’am, baise ayubu’umaim i nati bairi tama’am. Naatu Jesu wabinamaim orot yait nati sisinaf baibatiyen abitin, nati’imaim atama atao efanin iti’imaim ao.
4 Mukasonkhana mu dzina la Ambuye athu Yesu, ine ndili nanu mu mzimu, ndipo mphamvu ya Ambuye athu Yesu ili pomwepo,
4 Ata Regah Jesu Keriso wabinamaim a kou’ay kwabaib, ayu ayubu’umaim i nati wanawanamaim, naatu Regah ana fair ere etatargubi ana veya
5 mumupereke munthuyu kwa Satana, kuti chikhalidwe chake cha uchimo chiwonongedwe ndikuti mzimu wake udzapulumuke pa tsiku la Ambuye.
5 nati orot bowabow kakafin sisinaf i Satan kwanitin biyan ana kakafin nagurus, saise ata Regah nanan ana veya’amaim ayubin boro yawas nitin.
6 Kudziwa kwanu si kwabwino. Kodi simukudziwa kuti yisiti wochepa amafufumitsa mphumphu yaufa wonse wa tirigu?
6 Kwa taiyuw kwabobora’ara’ahi ana itinin men gewasin, tur hio i kwaso’ob. “Yeast kikimin maiyow, baise faraw wanawanan hinayai hinakakamat boro nara’at nagadid.”
7 Chotsani yisiti wakale kuti mukhale ndi mphumphu yopanda yisiti, monga inu muli. Pakuti Khristu, Mwana Wankhosa wa Paska wathu, anaperekedwa nsembe.
7 Yeast atamanin i kwaisaroun, saise kwa boro faraw boubun wanawanan ana yeast en kwanamatar, boun kwama’am na’atube kwanama. Anayabin Keriso Tar Nowaten ana sheep natun i sibor yai’ika.
8 Choncho, tiyeni tisunge chikondwererochi, osati ndi yisiti wakale, wowononga ndi woyipa, koma ndi buledi wopanda yisiti, buledi woona mtima ndi choonadi.
8 Isan imih Tar Nowaten ana hiyuw isan tanaben taniyasisir, men yeast atamaninamaim, anayabin yeast atamanin wanawanan i baiyow ana koukra’at naatu tafa’asar ema’am, baise faraw wanawanan yeast en, nati faraw i uhew naatu mamarin.
9 Ndakulemberani mʼkalata yanga kuti musayanjane nawo anthu achigololo.
9 Ayu au fef kwa isa akikirum i ao kwanowar, sabuw baiwa’an kwanekwaneyah men bairi kwanita’imon.
10 Pamenepatu sindikutanthauzatu anthu a dziko lapansi lino amene ndi achigololo, kapena aumbombo, kapena opeza ndalama mwachinyengo, kapena opembedza mafano. Kukanatero mukanangochoka mʼdziko lapansi lino.
10 Iti ao i men sabuw iyab baitumatum atih hima tibiwa’an kwanekwan, tibikabat, tebabain, naatu umataratar tekwakwafirih haiwih isan ao’omih. Baise sabuw nati na’atube haiwih isan kwa boro tafaram ana yawas tutufin etei kwanakwahir.
11 Koma tsopano ndikukulemberani kuti musayanjane ndi aliyense amene adzitcha mʼbale koma ndi wachigololo, kapena waumbombo, kapena wopembedza mafano, kapena wonamizira anzake, woledzera kapena wopeza ndalama mwachinyengo. Munthu wotere ngakhale kudya, osadya naye pamodzi.
11 Baise ayu ao i kwa taiyuw a sabuw baitumatumayah, iyab tibiwa’an kwanekwan, tibikabat, sawar umataratar tekwakwafirih, taituwah terararafih, tetomatom kwanekwan, tibifufuwen, i bairi men kwanaa kwanatom isan ao.
12 Kodi ndipindulanji kuti ndiweruze anthu amene si a mu mpingo? Kodi simuyenera kuweruza iwo amene ali mu mpingo?
12 Ayu men au ef ema’am boro ekaleisia sabuw tafaror ufunane tema’am ana fufunih, baise ana gewasin kwa i boro a kou’ayomaim taituwa akisihimo kwanibatiyih kwanayamutufurih.
13 Mulungu adzaweruza akunja. “Chotsani woyipayo pakati panu.”
13 God akisinamo sabuw iyab kou’ay ufunane tema’am boro nibatiyih. Buk Atamaninamaim eo na’atube, “Sabuw tafa’asarih a kou’ayomaim kwanunih titit.”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Coríntios 5, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.