1 Coríntios 4
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Choncho tsono anthu atione ife monga atumiki a Khristu, ndiponso ngati osunga zinsinsi za Mulungu.
1 Naatu boun it i Keriso ana akir wairafih na’atube sabuw hina’itit, naatu God ana buriburih koubuna’ayah na’atube hina’itit.
2 Chofunika kwambiri nʼchakuti amene apatsidwa udindo oyangʼanira aonetse kukhulupirika.
2 Naatu sabuw iyab hitutumih iti bowabow hibitih hai orot ukwarih isah hinabosunusunub.
3 Ine ndilibe nazo kanthu ngati ndiweruzidwa ndi inu kapena khothi lina lililonse. Ndithu, inenso sindidziweruza ndekha.
3 Ayu au yawas kwanafufun o sabuw au yawas hinafufufun isan men abiyababan. Anababatun a tur ao’owen taiyuwu au yawas men afufufun.
4 Chikumbumtima changa sichikunditsutsa, koma sikuti ndine wolungama. Wondiweruza ine ndi Ambuye.
4 Ayu taiyuw au not iu’uwu men kakafin ta asinaf, baise boro men nati’imaim anab au kakafin en ana’omih. Regah akisin boro ayu nibatiyu.
5 Chomwecho musaweruze nthawi yoweruza isanakwane. Dikirani mpaka Ambuye atabwera. Iye adzaonetsa poyera zimene zabisika mu mdima ndipo adzaonetsa maganizo a mʼmitima ya anthu. Pa nthawi imeneyo aliyense adzalandira kwa Mulungu chiyamiko.
5 Isan imih orot babin baibatiyin isan veya hiyai’iyai boro enan, kwanakaif Regah nan natitabo. I nanan ana veya gugumin wanawanan abisa wa’iwa’irin inu’in marakaw boro nakusisiar narun naatu orot dogoroh ana wa’iwa’irin etei boro nabow hinatit hinirerereb. Imaibo orot ta’ita’imon abisa hisisinaf isan God boro nabora’ara’ahih.
6 Tsono abale, ndapereka chitsanzo cha ine mwini ndi Apolo kuti mupindule. Phunzirani kwa ife tanthauzo la mawu akuti, “Musamapitirire zimene Malemba akunena,” kuti musamanyade pamene wina aposa mnzake.
6 Taitu, boun ayu akokok Apollos airi biyai’imaim bai’obaiyen ta anayai kwata’itin, saise tur abisa hio hikikirum yabin kwanaso’ob. “Tur abisa hikikirum ana fofoninamaim kwanao, men kwanatetebon.” Orot ta kwanabora’ah naatu ta kwananuw furuw kwanau kwaniyimih.
7 Pakuti ndani amakusiyanitsani ndi wina aliyense? Nʼchiyani muli nacho chimene simunalandire? Ndipo ngati munalandira, bwanji mumadzitukumula ngati kuti simunalandire?
7 Yait eo kwanowar kwa i turanah etei tafahimaim? Sawar etei kwabow kwama’ama etei i God it. Aisim taiyuw kwabobora’ara’ahi, ana itinin iti usar i kwabai kwaniyibe?
8 Inu muli nazo kale zonse zimene mufuna! Inu mwalemera kale! Inu mwayamba kale kulamulira ife! Ndilakalaka mukanakhaladi mafumu kuti ife tikhale nawo mafumu pamodzi ndi inu.
8 Kwa a kok sawar etei i kwabow karam kwama’am. Naatu boun kwa i totobuyoy wairaf kwamatar, kwana kwai’aiwoboka, aki baise en. Au notamaim akokok mi’itube kwati’aiwob gewas, saise aki auman bairit tati’aiwob youn.
9 Pakuti kwa ine zikuoneka ngati kuti Mulungu watiyika ife atumwi pachionetsero, kumapeto kwa mndandanda, monga anthu oweruzidwa kuti akaphedwe mʼmabwalo. Ife tayikidwa kuti tionekere ku dziko lonse, kwa angelo ndi anthu.
9 Ayu akisu au itinin, aki tur abarayah ai efan i urantoro’ot anababatun God yai, ana itinin dibur sabuw bebeyan ma’o’ow ana efanamaim terouw temomorob na’atube. Aki boro bebeyanamaim ana morob tounamatar naatu sabuw tutufin etei hinamau’uwi.
10 Ife ndife opusa chifukwa cha Khristu, koma inu ndinu anzeru mwa Khristu! Ife ndife ofowoka koma inu ndinu amphamvu! Inu ndinu olemekezeka koma ife ndife opeputsidwa!
10 Keriso wabinamaim taiyuwi ai’itinin na koko’awabe amatar, baise kwa i Keriso wanawananamaim kwana not wairafi kwamatar. Aki i ariririm, baise kwa a fair i erara’at, aki tinunuw furuwi, baise kwa i tekakakafiyi.
11 Mpaka pano tili ndi njala ndi ludzu, tili ndi sanza, tikuzunzidwa, tilibe nyumba.
11 Iti boun ana veya’amaim aki sikai harewamih mamah, abi’aamorob, ai ar ai faifuw tibiririk, segar hiborabirabi efamaim a’in ama areremor ai bar en.
12 Timagwira ntchito molimbika ndi manja athu. Akamatitemberera, ife timadalitsa; tikasautsidwa, ife timapirira.
12 Bowabow gagamin maiyow abowabow isan ahahahar, sabuw teo rarafi ana veya’amaim aki baigegewasin abitih, terabi tibia’akiri ana veya aki ewawainabi.
13 Pamene atilalatira timayankha mwachifundo. Mpaka pano takhala ngati zinyalala za dziko, monga zakudzala za dziko lapansi.
13 Tiu’uwi kwanikwaniyi ana veya, yabow turamaim abiyafutih. Boun ana veya’amaim aki i tafaram ana hain naatu bay ana merekas na’atube amatar.
14 Sindikulemba izi kuti ndikuchititseni manyazi, koma kukuchenjezani monga ana anga okondedwa.
14 Ayu iti fef i men kwa itinin biya’ohow isan akikirumamih. Baise akokok animatnuwi, anayabin kwa i ayu natunatu au yabow.
15 Ngakhale muli ndi anthu 10,000 okutsogolerani mwa Khristu, mulibe abambo ambiri, popeza mwa Khristu Yesu, ine ndakhala abambo anu kudzera mu Uthenga Wabwino.
15 Basit kwa ayub ana bonawiyenayah etei 10,000 na’atube tibi’obaiyi, baise tamatanah i men moumurih, anayabin Keriso Jesu ana baikofanamaim ayu ana kwa tamat amatar tur gewasin abai ana ait.
16 Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine.
16 Imih abifefeyani, ayu abisa asisinaf na’atube kwani’u’uru.
17 Chifukwa cha ichi ndikutumiza kwa inu Timoteyo, mwana wanga amene ndimamukonda, amene ndi wokhulupirika mwa Ambuye. Adzakukumbutsani inuyo za moyo wanga mwa Khristu Yesu, umene ukugwirizana ndi zimene ndimaphunzitsa paliponse mu mpingo uliwonse.
17 Ana’an iti isan ayu natu au yabow kek wabin Timothy kwa isa abiyafar. Iti kek i Regah ana bowabow isan ebobosunusunub, i enan boro kwa nuhinakusib, ayu au yawas naatu au bowabow mi’itube Keriso ana yawasamaim ama abowabow boro nao kwananowar, naatu mi’itube ekaleisia sabuw efan ta ta abi’obaiyih auman boro nao kwananowar.
18 Ena mwa inu mukudzitukumula, ngati kuti sindingabwere kwanu.
18 Kwa afa kwanotanot ayu boro men atan atinanawani kwarouw, imih kwa abai’oro’orot erara’at.
19 Koma ndibwera kwanuko posachedwapa, ngati Ambuye alola, ndipo ndi pamene ndidzadziwe osati zimene anthu odzitukumulawa akuyankhula, koma kuti mphamvu zawo nʼzotani.
19 Baise ayu boro’omo anan aninanawani, Regah nakokok na’at. Imaibo boro taiyuwu anaso’ob, naatu men bai’o’orotoyah hai tur akisin, baise hai fair menane hibaib auman anaso’ob.
20 Pakuti ufumu wa Mulungu si mawu chabe koma mphamvu.
20 Anayabin God ana aiwob i men turawat namomon, baise ana fair auman.
21 Kodi musankha chiyani? Kodi ndidzabwere ndi chikwapu, kapena mu chikondi ndiponso mwa mzimu wofatsa?
21 Kwa a kok i boro abisa anab anan kwana’itin? Wabir anab anan ana wabir? O taiyuwu ana yara’iyu yabowamaim anan kwa isa?
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Coríntios 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.