1 Coríntios 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Paulo, woyitanidwa mwachifuniro cha Mulungu kuti akhale mtumwi wa Khristu Yesu ndi mʼbale wathu Sositene.
1 Ayu Paul God ana kokomaim eafu atit Keriso Jesu ana Tur abarayan amatar taituwa Sosthenes airi.
2 Kupita ku mpingo wa Mulungu ku Korinto, kwa oyeretsedwa mwa Khristu Yesu ndi oyitanidwa kukhala opatulika ndiponso kwa onse amene amapemphera mʼdzina la Ambuye athu Yesu Khristu mʼdziko lonse lapansi, amene ndi Ambuye wawo ndi wathunso.
2 God ana Ekaleisia nati Corinth wanawanamaim kwama’am, iyabowat afa’af kwabai kwatit Keriso Jesu wanawananamaim kusouwi God ana sabuw kakafiyih kwamatar kwama’am, naatu sabuw efan tata’amaim iyabowat it bairit taikofan ata Regah Jesu Keriso wabinamaim tao takwakwafir auman.
3 Landirani chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye athu Yesu Khristu.
3 Manaw kabeber, tufuw, Tamat Godane naatu ata Regah Jesu Keriso’one kwa etei isa nama.
4 Nthawi zonse ndimayamika Mulungu chifukwa cha inu chifukwa cha chisomo chake chopatsidwa kwa inu mwa Khristu Yesu.
4 Ayu mar etei kwa isa God merarayow abitin, anayabin Keriso Jesu wanawananamaim God manaw kabeber bit isan.
5 Pakuti mwa Iye mwalemekezedwa mʼnjira iliyonse, mʼkuyankhula kwanu konse ndi mʼkudziwa kwanu konse,
5 Naatu i wanawananamaim kwa i kwana ef tata’ane totobuyoy wairaf kwamatar, a turamaim naatu not rerekabamaim sawar etei kwaso’ob.
6 chifukwa umboni wathu pa za Khristu unatsimikizidwa mwa inu.
6 Anayabin ayu Keriso isan ao’orereb i kwa wanawanamaim matar ebiturobe.
7 Choncho inu simusowa mphatso yauzimu iliyonse pamene mukudikira mofunitsitsa kuti Ambuye athu Yesu Khristu avumbulutsidwe.
7 Isan imih kwa ata Regah Jesu Keriso na bairerereb isan kwama kwakakaif wanawanan, men kafa’imo ayub ana baigegewasin ta kwasasa’irimih.
8 Adzakulimbikitsani mpaka kumapeto kuti mudzakhale wopanda mlandu pa tsiku lobwera Ambuye athu Yesu Khristu.
8 Naatu God boro nabototofari kwanan ana yomanin, saise ata Regah Jesu Keriso nanan ana Veya’amaim kwa boro aur ubar en na’iti.
9 Mulungu amene wakuyitanani inu mu chiyanjano ndi Mwana wake Yesu Khristu Ambuye athu ngokhulupirika.
9 God Natun ata Regah Jesu Keriso ana baita’ayomaim bairi run isan ea’afi i kwanitumitum.
10 Ndidandaulira inu, abale, mʼdzina la Ambuye athu Yesu Khristu kuti nonsenu muvomerezane wina ndi mnzake kuti pasakhale kugawikana pakati panu ndi kuti mukhale amodzi kwenikweni mu nzeru ndi mʼmaganizo.
10 Ata Regah Jesu Keriso ana roubabaruwen fair tafanamaim ayu abifefeyani taitu, abisa isan kwao’o etei kwanibasit, saise kwa wanawanamaim kouseb boro men nama, a not tutufin etei ta’imon namatar kwanama.
11 Abale anga, ena a ku nyumba ya Kloe andidziwitsa kuti pali mkangano pakati panu.
11 Taitu, ayu i Chloe tain tuwan afa hina, kwa wanawananamaim kwama kwabigamigam isan hio anowar.
12 Chimene ndikutanthauza ndi ichi: wina amati, “Ndimatsatira Paulo,” wina, “Ndimatsatira Apolo,” wina, “Ndimatsatira Kefa,” winanso, “Ndimatsatira Khristu.”
12 Ayu boro iti na’atube anao, kwa ta’ita’imon a tur ta ta kwao, o ta kuo, “Ayu i Paul abi’ufunun,” ta kuo, “Ayu Apollos abi’ufunun,” ta kuo, “Ayu Peter abi’ufunun,” naatu ta kuo, “Ayu i Keriso abi’ufunun.”
13 Kodi Khristu wagawikana? Kodi Paulo anapachikidwa pa mtanda chifukwa cha inu? Kodi munabatizidwa mʼdzina la Paulo?
13 Keriso i kwatarsisib in kau’ay nanabin matar. Iban Paul onaf afe’en kwa isa morob? Ai Paul bai’ufnuninamih bapataito kwabai?
14 Ine ndikuyamika kuti sindinabatizepo mmodzi mwa inu kupatula Krispo ndi Gayo,
14 Ayu God ana merar ayiy kwa men ta bapataito aitimih, Krisipas naatu Gaius hairi’imo,
15 mwakuti palibe amene anganene kuti anabatizidwa mʼdzina langa.
15 imih men yait ta boro inao, ayu i Paul wabinamaim bapataito abai abi’ufunun.
16 (Inde, ine ndinabatizanso a mʼbanja la Stefano, koma sindikumbukira ngati ndinabatizanso wina aliyense).
16 (Boro’obo anot Stephanas aawan ana nibur bairi bapataito aitih, baise anotanot men yait ta bapataito aitinimih.)
17 Pakuti Khristu sananditume ine kudzabatiza, koma kudzalalikira Uthenga Wabwino, osati ndi mawu anzeru za umunthu, kuopa kuti mtanda wa Khristu ungakhale wopanda mphamvu.
17 Anayabin Keriso i men bapataito isan iyafaru’umih, baise tur gewasin binan isan iyafaru, naatu men orot babin maiyow hai tur naatu hai notamaim ana’omih, nati na’atube ana’orerereb Keriso onaf afe’en momorob tur gewasin ana fair boro yabin en namatar.
18 Pakuti uthenga wa mtanda ndi chopusa kwa iwo amene akuwonongeka, koma kwa ife amene tikupulumutsidwa uthengawu ndi mphamvu ya Mulungu.
18 Anayabin onaf ana tur sabuw kasikasiyih isah i yabin en, baise iyabowat tayayawas isat i God ana fair
19 Pakuti kwalembedwa kuti,
19 Buk Atamaninamaim eo na’atube:
20 Munthu wanzeru ali kuti? Munthu wozama ndi maphunziro ali kuti? Munthu wodziwa zakuya zamakono ali kuti? Kodi Mulungu sanazipusitse nzeru za dziko lapansi?
20 Bo orot ukwarin rerekabin menamaim ema’am? Orot kirum so’obayan menamaim ema’am? Naatu orot baibasayan ana not gagamin iti tafaram nowan menamaim ema’am? God iti tafaram ana ukwar rerekab botabir na koko’aw mamatar men kwaso’ob?
21 Tsono poti mwa nzeru za Mulungu dziko lapansi mu nzeru zake silinamudziwe Iye, Mulungu amakondweretsedwa kuti kudzera mu chopusa cha zomwe zinalalikidwa apulumutse iwo amene akhulupirira.
21 Anayabin God ana ukwar rerekabamaim iwa’an sabuw tafaram ana ukwar rerekabamaim hima’am men karam boro hitaso’ob, naatu sabuw iyab iti tafaram ana ukwar rerekab hibaib, iti tur isan yabin en hirouw hio, baise aki onaf isan abibinanumaim God iti tur bai sinaf sabuw hitumatum yawas hibai.
22 Ayuda amafuna zizindikiro zodabwitsa ndipo Agriki amafunafuna nzeru,
22 Jew hikok ina’inan hita’itin hititurobe naatu Greek sabuw i ukwarerekab hinuwih.
23 koma ife timalalikira Khristu wopachikidwa. Chitsa chokhumudwitsa kwa Ayuda ndi chopusa kwa a mitundu ina.
23 Baise it i Keriso onaf afe’en hi’onaf momorob isan tabibinan, iti tur Jew sabuw tenonowar i tainih ekuyikuy, naatu Ufun Sabuw tenonowar isah i yabin en.
24 Koma kwa iwo amene Mulungu anawayitana, Ayuda ndi Agriki omwe, Khristu ndi mphamvu ya Mulungu ndi nzeru za Mulungu.
24 Baise Jew sabuw naatu Ufun Sabuw wanawanahimaim iyab God eafih hina yawas hibaib, nati sabuw isah Keriso i God ana fair naatu ana ukwar rerekab.
25 Pakuti za Mulungu zooneka ngati zopusa, ndi za nzeru kuposa nzeru za munthu, ndipo za Mulungu zooneka ngati zofowoka, zili ndi mphamvu kuposa mphamvu za munthu.
25 Anayabin God ana ukwar rerekab hi’itin koko’aw hirouw hio’o, i orot ana ukwar rerekab natabir, naatu God ana ririmin hi’itin hio’o, i orot ana fair natabir.
26 Abale taganizirani mmene munalili musanayitanidwe. Si ambiri a inu munali a nzeru, si ambiri a inu munali a mphamvu zamakopedwe. Si ambiri a inu munali obadwa pa ulemerero.
26 Taitu, kwa marasika mi’itube kwama’am ana maramaim God ea’afi i kwananot, sabuw hai itininamaim kwa moumur na’in i men not wairafi, men orot faifir, na’atube atufuwamaim men orot gagamih hai rara’ane kwatufuwamih.
27 Koma Mulungu anasankha zinthu zopusa za dziko lapansi kuti achititse manyazi anzeru. Mulungu anasankha zinthu zofowoka za dziko lapansi kuti achititse manyazi amphamvu.
27 Baise God tafaram ana sawar koko’aw hirarouw, rubinen sabuw not wairafih ibiya’uhuwih. Naatu tafaram ana sawar ririmih hirarouw rubinen, sabuw fairih ibiya’uhuwih.
28 Anasankha zinthu zapansipansi ndi zopeputsidwa za dziko la pansi lino, zinthu zimene kulibe, kuti asukulutse zimene zilipo,
28 Abisa tafaram itin yabin en rarouw i rubin bai, naatu abisa tafaram itin gagamin rarouw i gurus.
29 kuti munthu asanyade pamaso pa Mulungu.
29 Saise men yait ta God nanamaim naora’ara’atamih.
30 Nʼchifukwa cha Iye kuti inu muli mwa Khristu Yesu, amene wakhala nzeru ya kwa Mulungu, kwa ife, kunena kuti kulungama kwathu, chiyero ndi chipulumutso.
30 Baise God buwit tana Keriso Jesu wanawananamaim ikofanit naatu sinaf Keriso ata ukwar rerekab matar. Naatu kakafhine rufamit tatit, yamutufurit God ana sabuw kakafiyih tamatar.
31 Choncho poti zinalembedwa kuti, “Ngati munthu akufuna kunyadira, anyadire mwa Ambuye.”
31 Isan imih Buk Atamaninamaim eo na’atube, “Yait nakokok ora’ara’atamih Regah abisa sisinaf tafanamaim nao ra’ara’at.”

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Coríntios 1, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.