1 Coríntios 16

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Tsopano za zopereka zothandiza anthu a Ambuye a ku Yerusalemu. Muchite zomwe ndinawuza mipingo ya ku Galatiya kuti ichite.
1 Siwar God ana sabuw isah o’on baiyafarinamih kwao i boro ayu ekaleisia no Galasia’amaim sinafumih au’uwihibe kwanasinaf.
2 Pa tsiku loyamba la sabata lililonse, aliyense wa inu azipatula ndalama molingana ndi zomwe wapezera. Asunge, kuti ndikabwera pasadzakhalenso msonkhamsonkha.
2 Sunday ta’ita’imon kwa a mour ana fofonin kabay turin kwanayasaisir kwanita’ay, saise ayu ananan i boro men kabay tanao’onamih.
3 Pamenepo, ndikadzafika, ndidzawapatsa makalata a umboni anthu amene mudzawasankhe ndi kuwatuma kuti akapereka mphatso zanu ku Yerusalemu.
3 Ayu anan anatitit ana veya, orot iyab kwarubinih tema’am isah boro fef anakirum anitih naatu aniyafarih a siwar hinab hinan Jerusalem.
4 Ngati kutaoneka kuti nʼkoyenera kuti ndipite nawo, adzapita nane limodzi.
4 Ayu bairi namih hinanotanot na’at basit boro ayu hinakofanu bairi anan.
5 Ndidzafika kwanuko nditadutsa ku Makedoniya pakuti ndikuyembekezera kudzera ku Makedoniyako.
5 Ayu ufibo boro kwa isa anan, mat boro Masedonia anatit, anayabin ayu i Masedonia wanawananamaim remor isan ayayakitifuw.
6 Mwina ndidzakhala nanu kanthawi kochepa kapenanso nyengo yonse yozizira, kuti mudzandithandize kupitiriza ulendo wanga kulikonse kumene ndingapite.
6 Anotanot veya maninaka boro kwa bairit tanama, men aso’ob rarab siba’u tutufin etei boro tanama. Imaibo boro kwanibaisu au remor ana kofan maiye efan ta’amaim.
7 Sindikufuna kuti ndikuoneni tsopano mongodutsa chabe, koma ndikuyembekezera kudzakhala nanu kwa kanthawi, ngati Ambuye alola.
7 Ayu men akokok anan mar kafai bairi tanama naatu anihamiyi maiye anan, ayu akokok i boro anan veya maninaka bairit tanama, Regah nabibasit na’at.
8 Koma ndikhala ndili ku Efeso mpaka nthawi ya Pentekosite,
8 Baise ayu boro Ephesus imaim anama nanan Pentecost ana veya natit.
9 pakuti mwayi waukulu wapezeka woti nʼkugwira ntchito yaphindu, koma pali ambiri amene akutsutsana nane.
9 Anayabin bowabow anababatun ana etawan gagamin isou botawiy naatu sabuw moumurihika i ayu isou i mo’oh te’a’abar.
10 Ngati Timoteyo afike kwanuko, onetsetsani kuti pasakhale zina zomuchititsa mantha pamene ali pakati panu, pakuti iye akugwira ntchito ya Ambuye monga ine.
10 Timothy ef aumatan nanan biya natitit na’at ana merar kwanay saise biyan fari niwa’an, anayabin i Regah ana akir wairafin orot, ayu na’atube.
11 Wina aliyense asamunyoze. Muthandizeni kupitiriza ulendo wake mwamtendere kubwereranso kuli ine. Ndikumuyembekeza pamodzi ndi abale ena.
11 Men yait ta ina nuwfurubimih, baise kwanibais tufuwamaim ana remor nakofan nan, saise namatabir nan biyou natit. Anayabin ayu baitumatumayah afa bairi i ana matabir maiye isan ama anuwanuw.
12 Tsono kunena za mʼbale wathu, Apolo, ndinamuwumiriza kwambiri kuti abwere kwa inu abale, ndipo iye sanafune kupita tsopano. Koma akadzapeza mpata wabwino adzabwera.
12 Naatu taituwa Apollos isan mar bai’ab koufair aitin baitumatumayah afa bairi hitan hitananawani isan, nuhin tutufin men botabir boro boun ana veya’amaim tan, baise aren ta nabaib na’at boro nan.
13 Khalani tcheru; khazikikani mʼchikhulupiriro chanu; limbani mtima; khalani amphamvu.
13 Mata toniwa’an, baitumatumamaim kwanabatkikin, naatu kwana’abar totofar, kwanafair kwanabat.
14 Chitani zonse mwachikondi.
14 A bowabow etei yabowamaim kwanabow.
15 Mukudziwa kuti a mʼbanja la Stefano ndiye anali oyamba kutembenuka mtima ku Akaya, ndipo akhala akudzipereka kutumikira oyera mtima. Choncho ndikukudandaulirani, inu abale,
15 Kwa Stephanas aawan natunatun bairi isah i kwaso’obaka, Akaiya wanawananamaim i mat hina Kirisiyan himatar naatu taiyuwih hiyasairih hitit God ana sabuw isah hibow, isan taitu, kwa abifefeyani,
16 kuti muziwamvera anthu oterewa, ndiponso aliyense wogwira nawo ntchitoyi modzipereka.
16 bonawiyenayan sabuw iti na’atube i kwani’u’urih naatu sabuw iyabowat iti bowabow wanawanan hirun hikofanih bairi tebowabow auman.
17 Ndikondwera kuti Stefano, Fortunato ndi Akayiko afika, chifukwa akhala akundithandiza pakuti inu simuli nane.
17 Ayu i abiyasisir, Stephanas, Fotunatus naatu Akaikas hinan isan, anayabin kwa yumat aboboyouw efanin i hina ayu hibaisu.
18 Pakuti anatsitsimutsa mzimu wanga ndi wanu womwe. Anthu a mtundu oterewa ngofunika kuwalemekeza.
18 Naatu ayu au naniyan hikura’ah amisir, kwa hikukura’ahi na’atube. Sabuw iti na’atube i kwana’inanih a notamaim hinama.
19 Mpingo wa mʼchigawo cha ku Asiya ukupereka moni. Akula ndi Prisila akuperekanso moni wachisangalalo, mwa Ambuye, ndiponso mpingo umene umakumana mʼnyumba mwawo ukupereka moni.
19 Ekaleisia Asia tutufin wanawanan kwa a merar tiyiy, Aquila Priscilla hairi naatu ekaleisia iyabowat i hai baremaim bairi tibita’ay kwa a merar tiyiy Regah wabinamaim.
20 Abale onse kuno akupereka moni wawo. Patsanani moni wachikondi chenicheni.
20 Taituwa baitumatumayah etei iti’imaim tema’am kwa etei a merar tiyiy, naatu tufuw ana baimamamayen kwanimerarayowbonen kwanama.
21 Ineyo Paulo, ndikulemba ndi dzanja langa mawu awa akuti moni.
21 Ayu Paul taiyuwu umou’umaim iti a merarayow ana fef akirum abiyafar.
22 Ngati wina sakonda Ambuye akhale wotembereredwa. Maranatha! (Ambuye athu bwerani)!
22 Yait Regah men nabiyabuw, o rarafen tafanamaim nayen. “Maranatha,” Anayabin O Regah kuna.
23 Chisomo cha Ambuye Yesu chikhale ndi inu.
23 Ata Regah Jesu ana manaw ana kabeber mar etei biyamaim nama.
24 Chikondi changa chikhale ndi nonsenu mwa Khristu Yesu.
24 Keriso Jesu wanawananamaim kwama’am etei’imak abiyabuwi. Amen.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Coríntios 16, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.