1 Coríntios 15
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Tsono abale, ndikufuna ndikukumbutseni za Uthenga Wabwino umene ndinakulalikirani. Munawulandira ndipo munawukhulupirira kolimba.
1 Taitu, boun i akokok tur gewasin abinan kwanowar, imaim yawas kwabai, naatu imaim kwabatabatkikin isan nuhi akukusib.
2 Inu munapulumutsidwa ndi Uthenga Wabwinowu, ngati mwasunga mawu amene ndinakulalikirani. Kupanda kutero, mwangokhulupirira pachabe.
2 Iti tur gewasinamaim kwa iyawasi, imih tur abinan kwanonowar kwanabubukikin, baise men kwanabubukikin kwa a baitumatum boro nan yabin en namatar.
3 Pakuti chimene ndinalandira ndinapereka kwa inu monga chofunika kuposa zonse, kuti Khristu anafera zoyipa zathu monga mwa Malemba,
3 Ayu abisa abaib i kwa isa aya’abun, naatu nati tur ana’an gagamin i iti, Keriso it ata bowabow kakafin isan morob, Bukamaim eo na’atube.
4 kuti anayikidwa mʼmanda, kuti anaukitsidwa tsiku lachitatu monga mwa Malemba;
4 Hibai hin hubemaim hiyai, veya tounu ufunamaim misir maiye, Bukamaim eo na’atube.
5 ndipo kuti anaonekera kwa Petro, ndipo kenaka kwa Atumwi khumi ndi awiriwo.
5 Peter isan irerereb, imaibo tur abarayah nah 12 isah irerereb.
6 Pambuyo pake, Iye anaonekera kwa anthu oposa 500 mwa abale pa nthawi imodzi, ndipo ambiri mwa iwo akanali ndi moyo ngakhale kuti ena anagona tulo.
6 Nati ufunamaim veya ta’imon wanawanan ana bai’ufununayah etei 500 tafanamaim auman isah irerereb, moumurih na’in i boun yawasih tema’am baise afa i himorob.
7 Kenaka anaonekeranso kwa Yakobo, kenaka kwa atumwi onse.
7 Nati ufunamaim James isan irerereb, imaibo ana tur abarayah etei isah irerereb.
8 Potsiriza pa onse anaonekeranso kwa ine, monga mwana wobadwa nthawi isanakwane.
8 Uftoro’ot ayu atufuw kokobeya na’atube ama’am isou irerereb.
9 Pakuti ine ndine wamngʼono kwa atumwi ndipo sindiyenera nʼkomwe kutchedwa mtumwi chifukwa ndinazunza mpingo wa Mulungu.
9 Ayu i tur abarayah etei babahimaim imih ayu i men boro tur abarayan hinarouw hinao, anayabin God ana ekaleisia ai nununih arouw ai’a’akirih.
10 Koma mwachisomo cha Mulungu, ndili mmene ndililimu, ndipo chisomo chake kwa ine sichinali chopanda ntchito. Ndinagwira ntchito kuposa ena onse a iwo. Choncho sindine koma chisomo cha Mulungu chimene chinali ndi ine.
10 Baise God ana manaw ana kabeberamaim ayu tur abarayan amatar, naatu manaw kabeber ayu bitu i men yabin en, baise bowabow gagamin na’in abow, tur abarayah etei ana tabirih, men ayu au fairamaim abowabowamih, baise God ana manaw ana kabeber ayu wanawana’umaim ma ebowabow.
11 Tsono kaya ndi ineyo kapena iwowo, izi ndi zomwe timalalikira, ndipo izi ndi zimene munakhulupirira.
11 Isan imih i tibibinan naatu ayu abibinan ana itinin i men ta’amih, baise ana’an gagamin i abisa abibinan i kwa kwaitumatum.
12 Koma ngati timalalikira kuti Khristu anaukitsidwa kwa akufa, zikutheka bwanji kuti ena mwa inu azinena kuti kulibe kuuka kwa akufa?
12 Boun aki abibinan ai tur i Keriso morobone mimisir isan ao’o, baise mi’itube’emih kwa afa kwao moroboyah boro men hinayawas maiye hinamisir?
13 Ngati kulibe kuuka kwa akufa, ndiye kuti ngakhale Khristu sanaukenso.
13 Morobone misir maiye men nama’am na’at, ana itinin Keriso morobone men misir maiye’emih.
14 Ndipo ngati Khristu sanaukitsidwe, ndiye kuti kulalikira kwathu nʼkopanda ntchito, ndipo chikhulupiriro chanu nʼchopandanso ntchito.
14 Naatu Keriso morobone men tamimisir maiye na’at, aki ai binan i yabin en, naatu kwa Keriso kwabitumitum auman i yabin en.
15 Kuwonjezera pamenepa, ndiye kuti ndife mboni zabodza pa za Mulungu, pakuti tikuchita umboni kuti Mulungu anaukitsa Khristu kwa akufa. Ngati nʼzoona kuti akufa saukitsidwa, ndiye kuti Mulungu sanaukitsenso Khristu.
15 Naatu murumurubih men hinamimisir maiye na’at, aki i God isan abifufuwen. Anayabin Keriso morobone God baiyawasin arouw ao, naatu moroboyah morobone men hinamimisir maiye na’at, nati ebiturobe, God Keriso morobone men iyawas maiye misirimih.
16 Pakuti ngati akufa saukitsidwa, ndiye kuti nayenso Khristu sanaukitsidwe.
16 Morobone misir maiye men nama’am na’at, Keriso morobone men misir maiye.
17 Ndipo ngati Khristu sanaukitsidwe, chikhulupiriro chanu nʼchopanda ntchito; mukanali mu machimo anu.
17 Naatu Keriso morobone men tamimisir na’at, kwa a baitumatum i yabin en, naatu kwa i boro’ika bowabow kakafin tafatumi kwatama’ama.
18 Ndiye kuti nawonso amene agona tulo mwa Ambuye ndi otayika.
18 Naatu iban maiye sabuw iyab Keriso wabinamaim himomorob ana itinin i hikasiy na’atube.
19 Ngati kukanakhala kuti tili ndi chiyembekezo mwa Khristu mʼmoyo uno wokha, tikanakhala omvetsa chisoni kuposa anthu ena onse.
19 Keriso wanawananamaim yawas tabai nuhit fot tama’am. Baise ata yawas i iti tafaram akisin isan tanama tananotanot na’at. It i tafaram wananwanan ana gonenet sabuw tamatar.
20 Koma nʼzoonadi kuti Khristu anaukitsidwa kwa kufa, chipatso choyamba cha onse ogona tulo.
20 Baise turobe Keriso i anababatun morobone misir maiye, God ana sabuw iyab himomorob wanawanahimaim Keriso i wan morobone misir.
21 Pakuti monga imfa inadza kudzera mwa munthu, kuuka kwa akufa kwabweranso kudzera mwa munthu.
21 Anayabin orot ta’imon ana sinafumaim morob matar, imih orot ta’imon ana sinafumaim morobone misir maiye matar.
22 Pakuti monga mwa Adamu onse amafa, chomwechonso mwa Khristu onse adzakhala ndi amoyo.
22 Sabuw etei tamomorob, anayabin Adam ana rara, naatu morobone boro tanamisir maiye anayabin Keriso yawasin ema’am.
23 Koma aliyense adzauka pa nthawi yake. Khristu ndiye woyambirira, pambuyo pake, pamene Khristu adzabwera, iwo amene ali ake adzauka.
23 Baise morobone tanamimisir maiye, i boro koumutufuren inu’in na’atube hinabusuruf, wantoro’ot boro Keriso namisir, naatu nanan ana veya sabuw iyab Keriso nowan boro hinamisir.
24 Pamenepo chimaliziro chidzafika, pamene Iye adzapereka ufumu kwa Mulungu Atate, atathetsa ufumu wonse, ulamuliro wonse ndi mphamvu zonse.
24 Imaibo mar yomanin nan natit, tafaram hai bonawiyenenayah, hai aiwob, hai kaifenayah etei hai fair tutufin Keriso nagugurus ufunamaim, aiwob nab Tamah God nitin.
25 Pakuti Iye ayenera kulamulira mpaka Mulungu atayika pansi pa mapazi ake adani ake onse.
25 Naatu Keriso i boro ni’aiwob nanan ana rakit sabuw etei nabow nan an babanamaim nawastanen.
26 Mdani wotsiriza kuwonongedwa ndi imfa.
26 Naatu uftoro’ot i sawar wabin Morob it ata rakit gagamin boro nagurus nitaiy nare.
27 Pakuti Mulungu “wayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake.” Ponena kuti wayika “zinthu zonse pansi pa mapazi ake,” nʼchodziwikiratu kuti sakuphatikizapo ndi Mulungu yemwe, amene anayika zinthu zonse pansi pa Khristu.
27 Anayabin Buk Atamaninamaim eo, “Sawar etei boro nabow an babanamaim naya.” Iti tur Sawar etei an babanamaim yara’iyen rouw eo, i rerereb yan, God men i auman bobar eomih, anayabin God sawar etei boro Keriso ana fair babanamaim naya.
28 Pamene adzatsiriza kuchita zimenezi, Mwana weniweniyo adzakhala pansi pa ulamuliro wa Iye amene anayika zinthu zonse pansi pake, kuti Mulungu akhale zonse mu zonse.
28 Sawar hinabow hinan God Natun babanamaim hinaya’ay ufunamaim, Jesu boro Tamah God ana fair babanamaim namare, anayabin sawar etei God bow Natun babanamaim ya, naatu God boro sawar tutufin etei ni’ukwarin ana sabuw etei isah.
29 Tsono ngati kulibe kuuka kwa akufa, kodi iwo amene akubatizidwa chifukwa cha akufa, adzatani? Ngati akufa saukitsidwa nʼkomwe, bwanji nanga anthu akubatizidwa mʼmalo mwawo?
29 Naatu morobone misir maiye en na’at, sabuw iyab moroboyah efanih bapataito hibaib boro abistan hinasinaf? Naatu morobone misir maiye en na’at, aisim sabuw moroboyah efanih taih tuwah hina bapataito tebaib?
30 Ndipo kwa ife, tikuyikiranji moyo wathu pachiswe nthawi ndi nthawi?
30 Naatu it auman aisim ata yawas takwahir tatit veya matan tayi tabowabow?
31 Abale, ndimafa tsiku ndi tsiku, ndikunenetsa zimenezi, mongotsimikizira monga ndimakunyadirani mwa Khristu Yesu Ambuye athu.
31 Taitu ayu i mar etei morob ana efanamaim ama’am. Anayabin sawar abisa Keriso kwa isa sisinaf imaim ayu kura’ara’ahu iti tur akukurerereb.
32 Ngati ndinalimbana ndi zirombo za kuthengo ku Efeso pa zifukwa za umunthu chabe, ndapindulanji? Ngati akufa sadzaukitsidwa,
32 Morob ufunamaim yawas men tama’am, aisim ayu iti Ephesus hai sigarafor bairi atiyow? Abisa ana gewasin boro anab? Morobone misir maiye en na’at.
33 Musasocheretsedwe, “Kukhala mʼmagulu oyipa kumawononga makhalidwe abwino.”
33 Men sabuw hinifufuwi a not hinakwaris. “A ofonah kakafih boro ayawas gewasin hinagurus.”
34 Ganizani bwino monga kuyenerera, ndiye lekani kuchimwa; pakuti pali ena amene sadziwa Mulungu. Ndikunena izi kuti muchite manyazi.
34 Ukwar kwanabotawiy gewas, ef kakafih kwasisinaf kwanihamiyen, anayabin kwa afa God men kwaso’ob, iti ao, saise kwa biya hina’ohow.
35 Koma wina akhoza kufunsa kuti, “Kodi akufa amaukitsidwa motani? Adzauka ndi thupi la mtundu wanji?”
35 Sabuw afa boro hinibatiy hinao, “Moroboyah boro mi’itube hinamisir maiye? Naatu hina mimisir biyah ana itinin boro mi’itube hinab?”
36 Wopusa iwe! Chimene mudzala sichikhala ndi moyo pokhapokha chitayamba chafa.
36 Taitu, kwabikoko’aw, ub me yanamaim kutatanum boro men saife nakuboun nayenamih, baise wantoro’ot i boro namorob nare, imaibo nakuboun nayen.
37 Mukadzala, simudzala thupi limene lidzamere, koma mbewu chabe, mwina ya tirigu kapena ya china chake.
37 Naatu sanabey ub o ub afa kutatanum i men biyan tutufin kwatatanumimih, baise ro’on, sanabey ro’on o ub ta ro’on.
38 Koma Mulungu amayipatsa thupi monga Iye wafunira, ku mbewu ya mtundu uliwonse amapereka thupi lakelake.
38 God ub ta’ita’imon biyah hai itinin ta ta i ana kokomaim ya, naatu ub ta’ita’imon biyah anababatun itih.
39 Mnofu siwofanana. Anthu ali ndi mnofu wa mtundu wina, nyama zili ndi wina, mbalame zili ndi wina, nsomba zili ndi winanso.
39 Naatu sawar tafaramamaim biyah finimih auman hai itinin i men ta’imon, biyah i ta ta, orot babin biyah ana itinin ta, haru for biyah ana itinin ta, mamu hai itinin i ta naatu siy i hai itinin ta.
40 Palinso matupi akumwamba ndipo palinso matupi a dziko lapansi; koma ulemerero wa matupi akumwamba ndi wina, ndi wa matupi a dziko lapansi ndi winanso.
40 Naatu mar ana biyan itinin ibo ta, na’atube tafaram biyan itinin ibo ta. Baise biyat no mar nowan ana bonamanamarin itinin ibo ta, naatu biyat tafaram nowan ana bonamanamarin ibo itinin ta.
41 Dzuwa lili ndi ulemerero wake, ndipo pali ulemerero wina wa mwezi, palinso ulemerero winanso wa nyenyezi. Ulemerero wa nyenyezi ndi wosiyanasiyana.
41 Veya ibo ana bonamanamarin itinin ta, sumar ibo ana bonamanamarin itinin ta, naatu daman ibo hai bonamanamarin itinin ta, baise daman wanawanahimaim ta’ita’imoh ibo hai bonamanamarin ta ta.
42 Zidzaterenso pamene akufa adzauka. Thupi loyikidwa mʼnthaka ngati mbewu limavunda, koma likadzauka lidzakhala losavunda.
42 Baise Moroboyah hinamimisir maiye ana itinin i boro nati na’atube, biyat morob hubemaim tayayare ana veya biyat i emasamas, baise morobone namimisir ufunamaim boro nama wanatowan.
43 Limayikidwa mʼmanda mopanda ulemu, koma likadzaukitsidwa lidzakhala ndi ulemerero. Limayikidwa mʼmanda lili lofowoka, koma likadzaukitsidwa lidzakhala ndi mphamvu.
43 Biyat hubemaim tayayare itinin i kakafin, naatu siba’u’un, baise emimisir ana veya itinin i gewasin naatu fairin.
44 Limayikidwa mʼmanda thupi la mnofu chabe, koma likadzaukitsidwa lidzakhala lauzimu.
44 Biyat tayayare i tafaram nowan, baise emimisir i mar biyan.
45 Kwalembedwa kuti, “Munthu woyamba Adamu anakhala wamoyo,” Adamu wotsiriza anakhala wopatsa moyo.
45 Buk Atamaninamaim hikirum hio na’atube, “Orot wantoro’ot wabin Adam i biyan ana yawas bai,” baise Adam bairou’abin nan i ayubit ana yawas wanatowanin baitit isan na.
46 Zauzimu sizinabwere koyambirira, koma zachilengedwe, pambuyo pake zauzimu.
46 Orot ayubit ana yawas auman ma’am i men mat na, baise orot biyat ana yawasamaim ma’am i mat na, imaibo orot ayubit ana yawasamaim ma’am na.
47 Munthu woyamba anali wa dziko lapansi, wochokera mʼnthaka koma munthu wachiwiri anali wochokera kumwamba.
47 Orot wantoro’ot Adam i me nowan fofobane matar, baise Adam bairou’abin i marane ra’iy.
48 Monga analili munthu wa dziko lapansi, momwemonso anthu onse amene ndi a dziko lapansi. Ndipo monga alili munthu wakumwamba, momwemonso anthu onse amene ndi akumwamba.
48 Sabuw iyab me nowan biyah i orot me’emaim ma’am biyan na’atube, sabuw iyab mar nowan biyah i orot marane rara’iy biyan na’atube.
49 Ndipo monga momwe tinabadwa ofanana ndi munthu wa dziko lapansi uja, momwemonso tidzakhala ofanana ndi munthu wakumwamba.
49 Tafaram orot ana ana itinin tabaib na’atube, mar ana orot nanan ana itinin boro tanab.
50 Ndikunenetsa, abale, kuti thupi ndi magazi sizingathe kulowa mu ufumu wa Mulungu, ndipo zimene zimavunda sizingathe kulowa kumene zinthu sizivunda.
50 Taitu, abisa ao au yabin i iti, biyat, naatu finimit men karam boro God ana aiwobomaim narun, anayabin biyat i boro namorob namas, imih men karam boro wanatowan ma’am ana efanamaim narun.
51 Tamverani, ndikuwuzeni chinsinsi. Tonse sitidzagona tulo, koma tonse tidzasandulika.
51 Tain kwanarub gewas, iti tur buriburin anao kwananowar, it etei boro men tanamorobomih, baise ata itinin boro nabotabir bonamanamarin namatar
52 Zidzachitika mwadzidzidzi, mʼkamphindi kochepa, monga ngati kuphethira kwa diso, pa lipenga lotsiriza. Pakuti lipenga lidzalira, akufa adzaukitsidwa opanda chovunda, ndipo ife tidzasandulika.
52 tour natut ana veya namanamar ebowabow na’atube, tanimatanubamo biyat nabotabir. Anayabin tour natut ana veya murumurubih etei boro biyah fairin hinamisir, naatu biyah ana itinin boro nabotabir.
53 Pakuti chovunda chiyenera kuvala chosavunda, ndi thupi ili lakufa liyenera kuvala losafa.
53 Biyat iti morob emasamas boro nabotabir biyat fairin wanatowan ma’ama’anin namatar.
54 Pamene thupi lovundali likadzasanduka losavunda, ndipo thupi lotha kufali likadzasanduka losatha kufa, pamenepo zidzakwaniritsidwa zimene zinalembedwa zakuti, “Imfa yogonjetsedwa kwathunthu.”
54 Biyat iti boun tama’am boro namorob naatu namas, baise morob ufunamaim biyat boro nabotabir nan wanatowan ma’ama ana biyan nab. Imaibo Buk Atamaninamaim hikirum boro nan niturobe,
55 “Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti?
55 “Morob o a fair menanamaim ema’am boro inisnowah?
56 Ululu wa imfa ndi tchimo, ndipo mphamvu ya tchimo ndi lamulo.
56 Morob ana biyababan i bowabow kakafinane ebaib, naatu bowabow kakafin ana fair i ofafaramaim ebaib.
57 Koma tiyamike Mulungu amene amatipambanitsa mwa Ambuye athu Yesu Khristu.
57 Baise God ana merar tanay anayabin Jesu Keriso, i morob ana ahay ana waf tagagir yare!
58 Choncho, abale anga okondedwa imani njii. Musasunthike ndi chilichonse. Nthawi zonse mudzipereke kwathunthu ku ntchito ya Ambuye, chifukwa mukudziwa kuti ntchito zanu mwa Ambuye sizili zopanda phindu.
58 Isan imih taitu, yate nanub kwanabatkikin, mar etei Regah isan anot tutufin kwanabow, anayabin Regah isan kwabow kwabi’akir i men anayabin enamih, baise yabin auman.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Coríntios 15, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.