1 Coríntios 13
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI
1 Ngakhale nditamayankhula mʼmalilime a anthu ndi a angelo, koma ngati ndilibe chikondi, ndili ngati chinganga chaphokoso kapena ngati chitsulo chosokosera.
1 Ayu i karam boro menau nabotabir sabuw hai turamaim anao, o tounamatar hai tur anao, baise auru yabow en na’at, au tur ao i naniyan en ber terab etefotef na’atube.
2 Ngati ndili ndi mphatso ya uneneri, nʼkumazindikira zinsinsi ndi kudziwa zonse, ndipo ngati ndili ndi chikhulupiriro chosuntha mapiri, koma wopanda chikondi, ine sindili kanthu.
2 Naatu ayu i God biyanane tur abai ao’orereb, ayu i so’ob wairafu, tur wa’iwa’irih hai kirikirifot etei aso’ob, ayu i baitumatum auru karam oyaw anao na’uy ra’ah nan. Baise auru yabow en na’at, ayu i au yabin en.
3 Ngati ndipereka zanga zonse kwa osauka ndi kupereka thupi langa kuti alitenthe, koma ngati ndilibe chikondi, ine sindipindula kanthu.
3 Ayu karam au sawar etei yababan sabuw ana faramih naatu biyau ana kwahir siboromih hina’afun, baise auru yabow en na’at, ana gewasin boro men ta anab.
4 Chikondi nʼcholeza mtima, chikondi nʼchokoma mtima, chilibe nsanje, sichidzikuza, sichidzitamandira.
4 Yabow i yatenuban, yabow i koununub gewasin, yabow i men baibobowenayan, men bai’o’orotoyan, men ora’ara’atayan, men baitengogorayan,
5 Chikondi chilibe mwano, sichodzikonda, sichipsa mtima msanga, sichisunga mangawa.
5 yabow i men okwanekwaneyan, yabow men i taiyuwin ana gewasin enunuwetamih, men baiyaso’arayan, sabuw hai kakafih ana bukamaim men ekikirum,
6 Chikondi sichikondwera ndi zoyipa koma chimakondwera ndi choonadi.
6 yabow kakafin isan men ebiyasisir, baise turobe isan i ebiyasisir.
7 Chimatchinjiriza nthawi zonse, chimakhulupirika nthawi zonse, chimakhala ndi chiyembekezo nthawi zonse, chimapirira nthawi zonse.
7 Yabow i mar etei etatafafar, mar etei ebitumatum, mar etei nuhifotamaim ema’am, mar etei ebitafofor.
8 Chikondi ndi chosatha. Koma mphatso ya uneneri idzatha, pamene pali kuyankhula malilime adzatha, pamene pali chidziwitso chidzatha.
8 Yabow i ana yomanin en, dinabatur tao’orereb boro nasawar, menat ebotabir tur afa tao etei boro hinanutanub, abisa tasoso’ob etei boro nasisinasair.
9 Pakuti timadziwa zinthu pangʼono chabe ndipo timanenera pangʼono chabe.
9 Anayabin it i turinawat taso’ob, naatu dinabatur tur i turinawat tao’orereb. boro men tutufin tanaorereb nan yomanin tanisawarimih.
10 Koma changwiro chikadzaoneka ndipo chopereweracho chidzatha.
10 Baise koubaitotor ana veya nanan, sawar men koubatotoramaim ti’inu’in boro nasawar.
11 Pamene ndinali mwana ndinkayankhula ngati mwana, ndinkaganiza ngati mwana, ndinkalingalira ngati mwana. Koma nditakula, zonse zachibwana ndinazisiya.
11 Kek ana veya, kek hai tur ao, kek hai not anot, kek hai naniyanamaim ama, boun ana abi’orot ana veya, kek ana bowabow etei aihamiy.
12 Pakuti tsopano tiona zinthu mosaoneka bwino ngati mʼgalasi loonera; kenaka tidzaziona maso ndi maso. Tsopano ndidziwa mosakwanira koma kenaka ndidzadziwa mokwanira, monga mmene Mulungu akundidziwira ine.
12 Abisa boun ta’i’itin i men ta’i’inan gewas, anayabin kiyam matan sukwayan na’atube, imih God men tai’itin gewas, baise veya nanan, imaibo yumatan boro tana’itin naatu itabo yumatat na’itin. Naatu sawar tutufin etei boro tanaso’ob nan na’asa’ub, boun i turinawat taso’ob.
13 Ndipo tsopano zatsala zinthu zitatu: chikhulupiriro, chiyembekezo ndi chikondi. Koma chachikulu pa zonsezi ndi chikondi.
13 Naatu boun i sawar tounu tema’am, baitumatum, nuhifot, yabow, baise wanawanahimaim yabow i gagamin.
Atalhos do teclado
- Capítulo anterior←
- Próximo capítulo→
- Versículo anteriork
- Próximo versículoj
- Limpar seleçãoEsc
- Esta ajuda?
Estude este capítulo no WhatsApp
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Coríntios 13, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.