1 Coríntios 10

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA) vs AAI

Sair da comparação
AAI TUR GEWASIN O BAIBASIT BOUBUN
1 Pakuti sindikufuna kuti inu mukhale osadziwa zenizeni, abale, kuti makolo athu anatsogozedwa ndi mtambo ndikuti onse anawoloka nyanja.
1 Taitu, ata a’agir Moses nawiyih hititit ana veya abisa isah mamatar i kwananot. Ata a’agir etei rofom re tafafarih nawiyih Red Sea yan owasasin hirabon rewan rounane hiyen.
2 Ndipo onse anabatizidwa mwa Mose mu mtambo ndi mʼnyanja.
2 Rofom wanawanan naatu riy wanawanan hirarabon ana veya, etei bapataito hibai Moses ana bai’ufununayah himatar.
3 Onse anadya chakudya chimodzi chauzimu
3 Naatu Ayubih ana bay itinin ta’imon marane hire’er etei hibow hi’aa.
4 ndipo anamwa chakumwa chimodzi chauzimu; popeza anamwa kuchokera mʼthanthwe lomwe anayenda nalo, ndipo thanthwe limeneli linali Khristu.
4 Na’atube ayubit ana harew itinin ta’imon marane re’er etei hitom, naatu ayubit ana To’one harew tit hitomatom nawiyih bairi hin, nati to i Keriso taiyuwin.
5 Ngakhale zinali choncho, Mulungu sanakondwere ndi ambiri a iwo, motero ambiri mwa iwo anafera mʼchipululu.
5 Baise God ata a’agir moumurih na’in isah men iyasisir, imih himorob arar yan hai rarik awan karatan.
6 Tsono zinthu izi zinachitika kuti zikhale chitsanzo, kuti ife tisayike mitima yathu pa zinthu zoyipa monga anachitira makolo athuwo.
6 Naatu sawar iti himamatar i bai’obaiyen na’atube it isat, ebimatnuwit saise men kakafin sinafumih nakura’ara’ahit hisisinafube tanasinafumih.
7 Musakhale anthu opembedza mafano, monga analili ena mwa iwo. Pakuti zalembedwa kuti, “Anthuwo anakhala pansi nayamba kudya ndi kumwa. Kenaka anayimirira nayamba kuvina mwachilendo.”
7 Wagabur ata a’agir sawar iu’inuwih hikwakwafirih na’atube tanasinafumih. Buk Atamaninamaim iti na’atube eo “Sabuw himare hiyuw hi’aa hibiyasisir, hai yasisir botabir hitom hikoko’aw himisir hiwa’an kwanekwan.
8 Tisachite chigololo monga ena mwa iwo anachitira ndipo tsiku limodzi anafapo anthu 23,000.
8 Imih uwatanah afa hibiwa’an kwanekwanabe men taniwa’an kwanekwan, anayabin nati na’atube hisisinaf, veya ta’imon wanawanan sabuw etei 23,000 ah uy hire himorob.
9 Tisamuyese Khristu, monga ena mwa iwo anachitira ndipo anaphedwa ndi njoka.
9 Ata Regah men routobonamaim tanayai, uwatanah afa na’atube hisinaf Regah hirurutubun etei tuwamorob yubih himorob.
10 Ndipo osamawiringula, monga ena mwa iwo anachitira naphedwa ndi mngelo wowononga.
10 Men tanagam kwanekwan, anayabin afa na’atube hisisinaf gurugurusen ana tounamatar na etei rouw himorob.
11 Zinthu izi zinawachitikira kuti zikhale chitsanzo ndipo zinalembedwa kuti zikhale chenjezo kwa ife, amene tiyandikira nthawi ya kutha kwa zonse.
11 Sawar iti himamatar etei i bai’obaiyen na’atube it isat, naatu baimatnuwit isan bukamaim hikirum. Anayabin veya iti boun tama’ama i tana mar yomanin tatit.
12 Choncho, ngati mukuganiza kuti mwayima mwamphamvu, samalani mungagwe!
12 Imih o yait kunotanot i kubatabatkikin, inakaif gewas men inare’emih.
13 Palibe mayesero amene mwakumana nawo oposa amene anthu ena onse anakumana nawo. Mulungu ngokhulupirika; sadzalola kuti inu muyesedwe koposa muyeso umene mutha kupirira. Koma pamene mwayesedwa, Iyenso adzakupatsani njira yopambanira mayeserowo.
13 Routobon mar etei o kubaib na’atube, nati routobon ta’imon sabuw etei tebaib. Baise God ana omatanen mar etei ekakaif. Imih boro men nihamiy routobon gagamin inab a fair nanatabir a niyaweyaw inare’emih. Baise routobon inabaib ana veya i boro fair nit inabatkikin naatu ef nabotawiy inahaiw inatit.
14 Choncho abwenzi anga okondedwa, lekani kupembedza mafano.
14 Isan imih au ofonah, wagabur hai bowabow etei kwanihamiyen.
15 Ndikuyankhula kwa a anthu anzeru zawo, nokha muweruze pa zimene ndikunenazi.
15 Ayu iti tur i kwa not wairafi isa ao, saise au tur naniyan kwanab abisa ao kwana’itin.
16 Pamene tidalitsa chikho cha Mgonero wa Ambuye, mothokoza Mulungu, kodi sitikugawana magazi a Khristu? Nanga buledi amene timanyemayo, kodi sitikugawana thupi la Khristu?
16 Merarayow ana kerowas imaim God ana merar tayiy tatomatom ana veya, Keriso ana rara etei tafafaram. Naatu rafiy taimasib ta’ani’aan ana veya it etei’imak Keriso biyan tafafaram.
17 Pakuti buledi ndi mmodzi yekha, ifenso ngakhale tili ambiri, ndife thupi limodzi, popeza tonse timagawana buledi mmodzi yemweyo.
17 Anayabin rafiy fafar i ta’imon, it moumurit na’in, baise biyat i ta’imon, imih rafiy ta’imon tafafaram.
18 Taganizirani zimene amachita Aisraeli. Kodi onse amene amadya zoperekedwa nsembe, samachita nawo miyambo ya pa guwapo?
18 Israel sabuw hai sinaf i kwananot. Sheep tebow terouw gem tafanamaim tisibor finimih turih tefaram ta’aau i God bairi nati’imaim tibita’imon maiye.
19 Kodi ndikutanthauza kuti nsembe zoperekedwa kwa mafano ndi kanthu konse, kapena kuti mafano ndi kanthu konse?
19 Men kwananot ayu nati wagabur naatu sibor nati wagabur isah kwasisibor i abibasit kwanarouw.
20 Ayi. Nsembe za osakhulupirira zimaperekedwa kwa ziwanda, osati kwa Mulungu, ndipo sindikufuna kuti muziyanjana ndi ziwandazo.
20 En! Baise, abisa au’uwi ana’an i iti na’atube. Eteni Sabuw hai sibor i wagabur isah tisisibor, men God isan. Imih ayu men akok kwa wagabur bairi kwanikofan.
21 Simungamwe chikho cha Ambuye, ndi kukamweranso chikho cha ziwanda. Simungadyere pa tebulo la Ambuye ndiponso la ziwanda.
21 Kwa men karam boro Regah ana kerowasamaim kwanatom, naatu iban maiye wagabur hai kerowasimaim kwanatom. Naatu men karam Regah ana gem kakafiyinamaim kwanaa, naatu wagabur ana gem tafanamaim kwanaa maiye.
22 Kodi tikufuna kuwutsa mkwiyo wa Ambuye? Kodi ndife amphamvu kuposa Iye?
22 Men tanasinaf Regah ana yaso’ar tanakura’ahimih. Kwanotanot it Regah ana fair tanatabir? En!
23 Mutha kunena kuti, “Zinthu zonse nʼzololedwa,” komatu si zonse zili za phindu. “Zinthu zonse nʼzololedwa,” komatu si zonse zimathandiza.
23 Sawar etei i sinaf isan hibasit, baise sawar etei boro men ta ana gewasin nitimih. Naatu sawar etei i sinaf isan hibasit, baise sawar etei boro men hinibaisimih.
24 Munthu aliyense asafunefune zokomera iye yekha, koma zokomeranso ena.
24 Men yait ta akisin ana gewasin nanuwetamih, baise taituwan hai gewasin nanuwet.
25 Idyani nyama iliyonse imene amagulitsa pa msika, osafunsa mafunso okhudzana ndi chikumbumtima chanu.
25 Ahar efanamaim masanuw kwanatotobon kwana’aamo, men anot hinamour kwanibatebatemih.
26 Popeza kuti, “Dziko lapansi ndi la Ambuye ndi zonse za mʼmenemo ndi zake.”
26 Anayabin Buk Atamaninamaim iti na’atube eo, “Me yan sawar tutufin etei tema’am i Regah nowan.”
27 Ngati wosakhulupirira akuyitanani kuti mukadye naye, inuyo ndi kuvomera kupitako, mukadye chilichonse chimene akakupatseni ndipo musakafunse mafunso okhudzana ndi chikumbumtima chanu.
27 Orot baitumatum atin nifefeyani airi bay aamih kwanamare abisa namaim nayayare ina’aan, men anot hinamour inibatebatemih.
28 Koma ngati wina akuwuzani kuti, “Izi zaperekedwa nsembe,” musadye zimenezo, pofuna kuthandiza amene wakuwuzaniyo komanso chifukwa cha chikumbumtima.
28 Baise orot ta tainimaim na’afare nao, “Iti bay i wagabur isah hisibor.” Nati bay men ina’aan, orot eo’otani i inakakafiy anayabin masanuw ina’ani’aan boro inasinaf kakaf.
29 Ndikunena za chikumbumtima cha winayo osati chanu. Tsono mungafunse kuti, nʼchifukwa chiyani ufulu wanga ukuphwanyidwa chifukwa cha chikumbumtima cha munthu wina?
29 Nati i men o kakafin kusisinafumih, baise orot nati eo’otani na’iti boro o kakafin sinaf narouw nao. Aisim boro ayu au roufamen abaib sabuw afa hai notamaim ayu hinafufunu?
30 Ngati ndikuyamika Mulungu chifukwa cha chakudya, nanga munthu angandinyoze bwanji pa zinthu zomwe ndayamikira nazo Mulungu?
30 “Ayu au bay isan God aifefeyan igegewasin abai ani’aan, aisim sabuw boro au bay abigegewasin isan kakafin hinarouw hinao?”
31 Nʼchifukwa chake chilichonse mungadye kapena kumwa, kapena chimene mungachite, chitani zonse ku ulemerero wa Mulungu.
31 Imih abisa ku’ani’aan o kutomatom o kusisinaf etei God wabin bora’ara’ahin isan inasinaf.
32 Musakhumudwitse aliyense, kaya ndi Myuda, Mgriki, kapena mpingo wa Mulungu.
32 Jew sabuw, Greek sabuw, na’atube ekaleisia sabuw wanawanahimaim men yait ta iniwa’an yababan nab nare’emih.
33 Mu zonse ndikuyesetsa kukondweretsa aliyense mʼnjira iliyonse. Popeza sindikufunafuna zokondweretsa ine ndekha koma zokomera ambiri kuti apulumutsidwe.
33 Ayu i mar etei asisinaftobon sabuw afa aniyasisirih, saise anibaisih yawas hinab, men ayu taiyuwu aniyasisiru.

Ler em outra tradução

Comparar com outra

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar 1 Coríntios 10, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.