Salmos 8

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Inu Yehova Ambuye athu,

2 Kuchokera mʼkamwa mwa ana ndi makanda,

3 Pamene ndilingalira za mayiko anu akumwamba,

4 munthu ndani kuti Inu mumamukumbukira,

5 Inu munamupanga kukhala wocheperapo kusiyana ndi zolengedwa zakumwamba

6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu;

7 nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi

8 mbalame zamlengalenga

9 Inu Yehova, Ambuye athu,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 8, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.