Salmos 67

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

2 Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

3 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

4 Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

5 Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

6 Nthaka yabereka zokolola zake;

7 Mulungu atidalitse

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 67, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.