Salmos 63

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga,

2 Inu ndinakuonani ku malo anu opatulika

3 Chifukwa chikondi chanu

4 Ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga,

5 Mudzakhutitsa moyo wanga ndi zonona.

6 Pa bedi panga ndimakumbukira inu;

7 Chifukwa ndinu thandizo langa,

8 Moyo wanga umakangamira Inu;

9 Iwo amene akufunafuna moyo wanga adzawonongedwa;

10 Iwo adzaperekedwa ku lupanga

11 Koma mfumu idzakondwera mwa Mulungu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 63, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.