Salmos 52

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu?

2 Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena;

3 Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi.

4 Umakonda mawu onse opweteka,

5 Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya:

6 Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha;

7 “Pano tsopano pali munthu

8 Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi

9 Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 52, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.