Salmos 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Inu Yehova, achulukadi adani anga!

2 Ambiri akunena za ine kuti,

3 Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza,

4 Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula

5 Ine ndimagona ndi kupeza tulo;

6 Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene

7 Dzukani, Inu Yehova!

8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 3, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.