Salmos 17

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Imvani Inu Yehova pempho langa lachilungamo;

2 Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu;

3 Ngakhale Inu mutafufuza mtima wanga ndi kundisanthula usiku,

4 Kunena za ntchito za anthu,

5 Mayendedwe anga akhazikika pa njira zanu;

6 Ine ndikuyitana Inu, Mulungu wanga, pakuti mudzandiyankha;

7 Onetsani kudabwitsa kwa chikondi chanu chachikulu,

8 Mundisunge ine ngati mwanadiso;

9 kuchoka kwa oyipa amene amandizinga ine,

10 Iwo amatseka mitima yawo yopanda chifundo,

11 Andisaka, tsopano andizungulira

12 Iwo ali ngati mkango wofuna nyama;

13 Dzukani Yehova, mulimbane nawo ndipo muwagwetse pansi;

14 Inu Yehova, pulumutseni ndi dzanja lanu kwa anthu otere,

15 Ndipo ine mʼchilungamo ndidzaona nkhope yanu;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 17, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.