Salmos 132

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Inu Yehova, kumbukirani Davide

2 Iye analumbira kwa Yehova

3 “Sindidzalowa mʼnyumba mwanga

4 sindidzalola kuti maso anga agone,

5 mpaka nditamupezera malo Yehova,

6 Zoonadi, tinamva za Bokosi la Chipangano ku Efurata,

7 “Tiyeni tipite ku malo ake okhalamo;

8 ‘Dzukani Yehova, ndipo bwerani ku malo anu opumulira,

9 Ansembe anu avekedwe chilungamo;

10 Chifukwa cha Davide mtumiki wanu,

11 Yehova analumbira kwa Davide,

12 ngati ana ako azisunga pangano langa

13 Pakuti Yehova wasankha Ziyoni,

14 “Awa ndi malo anga opumapo ku nthawi za nthawi;

15 Ndidzadalitsa mzindawu ndi zinthu zambiri;

16 Ndidzaveka ansembe ake chipulumutso,

17 “Pano ndidzachulukitsa mphamvu za Davide

18 Ndidzaveka adani ake manyazi,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 132, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.