Salmos 12

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;

2 Aliyense amanamiza mʼbale wake;

3 Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo

4 Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;

5 “Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu

6 Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro

7 Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo

8 Oyipa amangoyendayenda ponseponse

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 12, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.