Salmos 116

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga;

2 Pakuti ananditchera khutu,

3 Zingwe za imfa zinandizinga,

4 Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova:

5 Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama

6 Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima;

7 Pumula iwe moyo wanga,

8 Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa,

9 kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova

10 Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati,

11 Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati,

12 Ndingamubwezere chiyani Yehova,

13 Ndidzakweza chikho cha chipulumutso

14 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova

15 Imfa ya anthu oyera mtima

16 Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu:

17 Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu

18 Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova

19 mʼmabwalo a nyumba ya Yehova,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 116, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.