Salmos 100

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.

2 Mulambireni Yehova mosangalala;

3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.

4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko

5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 100, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.