1 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Mulambireni Yehova mosangalala;
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;
Você se identifica como:
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)
1 Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Mulambireni Yehova mosangalala;
3 Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
4 Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
5 Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;
Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Salmos 100, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.
Uma mensagem curta de manhã, com um versículo para meditar — direto no seu celular. Sem propaganda.