Miquéias 2

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Tsoka kwa amene amakonzekera chiwembu,

2 Amasirira minda ndi kuyilanda,

3 Nʼchifukwa chake Yehova akuti,

4 Tsiku limenelo anthu adzakuchitani chipongwe;

5 Nʼchifukwa chake simudzakhala ndi munthu mu msonkhano wa Yehova

6 Aneneri awo amanena kuti, “Usanenere!

7 Inu nyumba ya Yakobo, monga zimenezi ndi zoyenera kuzinena:

8 Posachedwapa anthu anga andiwukira

9 Mumatulutsa akazi a anthu anga

10 Nyamukani, chokani!

11 Ngati munthu wabodza ndi wachinyengo abwera nʼkunena kuti,

12 “Inu banja la Yakobo, ndidzakusonkhanitsani nonse;

13 Amene adzawapulumutse adzayenda patsogolo pawo;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Miquéias 2, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.