Jó 25

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,

3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?

4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?

5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,

6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Jó 25, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.