Isaías 58

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 “Fuwula kwambiri, usaleke.

2 Pakuti tsiku ndi tsiku amafunafuna Ine;

3 Anthu akufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani ife tasala

4 Mumati uku mukusala kudya, uku mukukangana ndi kumenyana,

5 Kodi kusala kudya kumene ndimakufuna Ine nʼkumeneku,

6 “Kodi si uku kusala kudya kumene Ine ndimakufuna:

7 Anthu anjala kodi mwawagawira chakudya chanu?

8 Mukatero chipulumutso chanu chidzabwera ngati mʼbandakucha,

9 Mukamadzapemphera Yehova adzakuyankhani;

10 Ndipo ngati mudyetsa anthu anjala,

11 Yehova adzakutsogolerani nthawi zonse;

12 Anthu ako adzamanganso nyumba zimene zakhala mabwinja nthawi yayitali,

13 “Muzisunga osaphwanya Sabata;

14 mukatero mudzapeza chimwemwe mwa Yehova,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 58, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.