Isaías 51

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 “Mverani Ine, inu amene mukufuna chipulumutso

2 taganizani za Abrahamu, kholo lanu,

3 Yehova adzatonthozadi Ziyoni,

4 “Mverani Ine, anthu anga:

5 Ndili pafupi kubwera kudzawombola anthu anga.

6 Kwezani maso anu mlengalenga,

7 “Mverani Ine, inu amene mukudziwa choonadi,

8 Pakuti njenjete idzawadya ngati chovala;

9 Dzambatukani, dzambatukani! Valani zilimbe,

10 Kodi sindinu amene munawumitsa nyanja yayikulu,

11 Anthu amene Yehova anawawombola adzabwerera

12 Yehova akuti, “Ndinetu amene ndimakutonthozani mtima.

13 Koma inu mumayiwala Yehova Mlengi wanu,

14 Amʼndende adzamasulidwa posachedwa;

15 Pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu,

16 Ndayika mawu anga mʼkamwa mwanu

17 Dzambatuka, dzambatuka!

18 Mwa ana onse amene anabereka,

19 Mavuto awiriwa akugwera iwe.

20 Ana ako akomoka;

21 Nʼchifukwa chake imva izi iwe amene ukuvutika,

22 Ambuye Yehova wanu,

23 Ndidzapereka chikhocho kwa anthu amene amakuzunza,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 51, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.