Isaías 49

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Mverani Ine, inu anthu a pa zilumba

2 Iye anasandutsa pakamwa panga kukhala ngati lupanga lakuthwa,

3 Iye anati kwa ine, “Ndiwe mtumiki wanga, Israeli.

4 Koma Ine ndinati, “Ine ndinkaganiza kuti ndinagwira ntchito

5 Yehova anandiwumba ine

6 Yehovayo tsono akuti,

7 Yehova Mpulumutsi ndi Woyerayo wa Israeli akuyankhula,

8 Yehova akuti,

9 Ndidzawuza a mʼndende kuti atuluke

10 Iwo sadzamva njala kapena ludzu,

11 Mapiri anga onse ndidzawasandutsa njira yoyendamo,

12 Taonani, anthu anga adzachokera kutali,

13 Imbani mwachimwemwe, inu zolengedwa zamlengalenga;

14 Koma Ziyoni anati, “Yehova wandisiya,

15 “Kodi amayi angathe kuyiwala mwana wawo wakubere

16 Taona, ndakulemba iwe mʼzikhantho zanga;

17 Amisiri odzakumanganso akubwerera mofulumira,

18 Kweza maso ako ndipo uyangʼaneyangʼane

19 “Ngakhale unasanduka bwinja ndi kuwonongedwa

20 Ana obadwa nthawi yako yachisoni

21 Tsono iwe udzadzifunsa kuti,

22 Zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi,

23 Mafumu adzakhala abambo wongokulera

24 Kodi mungathe kulanda anthu ankhondo zofunkha zawo,

25 Koma zimene Yehova akunena ndi izi,

26 Anthu amene anakuponderezani adzadya mnofu wawo omwe;

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 49, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.