Isaías 27

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Tsiku limenelo,

2 Tsiku limenelo Yehova adzati,

3 Ine, Yehova, ndimawuyangʼanira;

4 Ine sindinakwiye.

5 Koma ngati apo ayi, abweretu kwa Ine adani angawo kuti ndidzawateteze;

6 Masiku akubwerawo Yakobo adzazika mizu,

7 Kodi Yehova anakantha Israeli

8 Yehova mwawalanga powapirikitsa ndi kuwatumiza ku ukapolo,

9 Yehova adzakhululuka kulakwa kwa Yakobo.

10 Mzinda wamalinga uja wasanduka bwinja,

11 Pamene nthambi za mitengoyo zauma, zimathyoka

12 Tsiku limenelo Yehova adzasonkhanitsa pamodzi anthu ake mmodzimmodzi kumalo opunthira tirigu, kuchokera ku mtsinje wa Yufurate mpaka ku mtsinje wa ku Igupto.

13 Ndipo tsiku limenelo lipenga lalikulu lidzalira. Amene akuzunzika ku Asiriya iwo amene ali ku ukapolo ku Igupto adzabwera ndi kudzalambira Yehova pa phiri lopatulika mu Yerusalemu.

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 27, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.