Isaías 15

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Uthenga wonena za Mowabu:

2 Anthu a ku Diboni akupita ku nyumba ya milungu yawo,

3 Mʼmisewu akuvala ziguduli;

4 Anthu a ku Hesiboni ndi Eleali akulira mofuwula,

5 Inenso ndikulirira Mowabu;

6 Madzi a ku Nimurimu aphwa

7 Kotero kuti chuma chomwe anachipeza ndi kuchisunga,

8 Kulira kwawo kukumveka mʼdziko lonse la Mowabu;

9 Madzi a ku Dimoni afiira ndi magazi,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Isaías 15, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.