Ezequiel 19

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 “Imba nyimbo ya madandawulo, kuyimbira akalonga a ku Israeli.

2 Uzinena kuti,

3 Unalera mmodzi mwa ana ake,

4 Anthu amitundu anamva za mkangowo,

5 “ ‘Amayi aja ataona kuti mwana ankamukhulupirira uja wagwidwa ndi kuti chiyembekezo chake chapita padera,

6 Unkayendayenda pakati pa mikango inzake,

7 Unagwetsa malinga awo,

8 Pamenepo mitundu ya anthu, makamaka ochokera madera ozungulira,

9 Anawukoka ndi ngowe nawuponya mʼchitatanga.

10 “ ‘Amayi ako anali ngati mpesa mʼmunda wamphesa

11 Nthambi zake zinali zolimba,

12 Koma unazulidwa mwaukali

13 Ndipo tsopano anawuwokeranso ku chipululu,

14 Moto unatulukanso mu mtengomo

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Ezequiel 19, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.