Amós 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (NYA)

1 Imvani mawu awa, inu ngʼombe zazikazi za ku Basani, okhala pa Phiri la Samariya,

2 Ambuye Yehova, mwa kuyera mtima kwake walumbira kuti,

3 Mudzatulukira mʼmingʼalu ya pa khoma

4 “Bwerani ku Beteli mudzachimwe;

5 Wotchani buledi wokhala ndi yisiti ngati nsembe yachiyamiko

6 “Ndine amene ndinakusendetsani milomo mʼmizinda yanu yonse,

7 “Ndinenso amene ndinamanga mvula

8 Anthu ankayenda mzinda ndi mzinda kufuna madzi,

9 “Nthawi zambiri ndinakantha mbewu zanu ndiponso minda ya mpesa,

10 “Ine ndinabweretsa miliri pakati panu

11 “Ndinawononga ena mwa inu

12 “Choncho izi ndi zimene ndidzakuchitire iwe Israeli,

13 Iye amene amawumba mapiri,

Ler em outra tradução

Comparar lado a lado

Estude este capítulo no WhatsApp

Peça à IA da Bíblia Fala para explicar Amós 4, comparar traduções ou montar um estudo — tudo direto pelo WhatsApp.